46
KUKHAZIKITSIDWA 1 …ine ndikumverera bwino kumva zimenezo, izo ndi zabwino. Chabwino, zimakhala chomwecho nthawizonse, monga ine ndanenerapo kale, “Ine ndinali wokondwa pamene iwo anati kwa ine, ‘Tiyeni tipite kunyumba ya Ambuye.’” Ine ndikukhulupirira Davide ananenapo zimenezo nthawiina, “Tiyeni tipite kunyumba ya Ambuye.” Ine sindikudziwa malo abwino aliwonse oti nkukakhalako, sichoncho inu, kuposa kukhala mnyumba ya Ambuye. 2 Tsopano, usikuuno, ife tiri ndi abwenzi ena pano amene achokera komwe ku Georgia. Iwo mwinamwake akhala akuyendetsa kupita kumusi tikatsiriza—tikatsiriza kudya chakudya cha masana usikuuno. Ndiyeno ife ti…Ena a iwo akuchokera kumusi uko, ine ndikudalira kuti mutsalira. Ndipo zipinda zimene ife tiri nazo ndi zotseguka kwa inu. 3 Ndipo kenako Lachitatu usiku ife tidzakhala tikupitirira, pa kuphunzira, ndipo kenako, Ambuye akalola, Lamlungu lotsatira kenanso. 4 Ndipo kenako Chautauqua adzayamba pa sikisi. Chotero nonse amene mwakonzekera tchuthi chanu, ife tikuyembekeza kuti tikakhala ndi nthawi yopambana, yodabwitsa ku Chautauqua. Kumeneko ndi kumene ife nthawizonse timakhala ndi nthawi yopambana yotero. Si magulu aakulu kwambiri, omwe nthawizina timakhala nawo…Umo mumakhala pafupifupi…Ine ndikuganiza ife tikhoza kuyikamo teni sauzande mmenemo, mophweka. Koma, kawirikawiri, chaka chatha ine ndikuganiza ife tinali ndi pafupifupi seveni sauzande, chinachake monga choncho. Malowo anali atadzadza, koma panali malo ambiri oti nkuimapo. Ndi mipando imene iwo akanakhoza kuyiyala mpaka panja. Ndipo chotero ife tikuyembekezera zimenezo. 5 Ndipo wokondwa kuwona ambiri a abale athu otumikira mkati muno. Ine ndikulephera kuti ndiganizire dzina lake apa, wamishonare, M’bale Humes ndi Mlongo Humes, kodi ndinu mwakhala pomwe apa, ndi ana, ndife okondwa kukhala nawo iwo, amishonare. Enawo, M’bale Pat, M’bale Daulton, ndi, oh, ambiri basi, M’bale Beeler. Ndipo ndinamuwona M’bale Collins mphindi pang’ono zapitazo. Ndipo, oh, izo zingakhale zovutirapo kuwatchula iwo onse. Koma ndife okondwa kwambiri kukhala nanu inu mnyumba ya Ambuye usikuuno. M’bale Neville wofunika wopambana uyu wakhala kumbuyo kwanga kuti azipemphera nane pamene ife tikhale tikuphunzitsa Mawu. Charlie, ndine wokondwa kukuwona iwe ndi Mlongo Nellie pano usikuuno, ana. Ichi ndi…ndipo

CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

  • Upload
    others

  • View
    0

  • Download
    0

Embed Size (px)

Citation preview

Page 1: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1

…ine ndikumverera bwino kumva zimenezo, izo ndizabwino. Chabwino, zimakhala chomwecho nthawizonse,

monga ine ndanenerapo kale, “Ine ndinali wokondwa pameneiwo anati kwa ine, ‘Tiyeni tipite kunyumba ya Ambuye.’”Ine ndikukhulupirira Davide ananenapo zimenezo nthawiina,“Tiyeni tipite kunyumba ya Ambuye.” Ine sindikudziwa maloabwino aliwonse oti nkukakhalako, sichoncho inu, kuposakukhala mnyumba ya Ambuye.2 Tsopano, usikuuno, ife tiri ndi abwenzi ena pano ameneachokera komwe ku Georgia. Iwo mwinamwake akhalaakuyendetsa kupita kumusi tikatsiriza—tikatsiriza kudyachakudya cha masana usikuuno. Ndiyeno ife ti…Ena a iwoakuchokera kumusi uko, ine ndikudalira kuti mutsalira. Ndipozipinda zimene ife tiri nazo ndi zotseguka kwa inu.3 Ndipo kenako Lachitatu usiku ife tidzakhala tikupitirira, pakuphunzira, ndipo kenako, Ambuye akalola, Lamlungu lotsatirakenanso.4 Ndipo kenako Chautauqua adzayamba pa sikisi. Choterononse amene mwakonzekera tchuthi chanu, ife tikuyembekezakuti tikakhala ndi nthawi yopambana, yodabwitsa kuChautauqua. Kumeneko ndi kumene ife nthawizonse timakhalandi nthawi yopambana yotero. Si magulu aakulu kwambiri,omwe nthawizina timakhala nawo…Umo mumakhalapafupifupi…Ine ndikuganiza ife tikhoza kuyikamo tenisauzande mmenemo, mophweka. Koma, kawirikawiri, chakachatha ine ndikuganiza ife tinali ndi pafupifupi sevenisauzande, chinachake monga choncho. Malowo anali atadzadza,koma panali malo ambiri oti nkuimapo. Ndi mipando imeneiwo akanakhoza kuyiyala mpaka panja. Ndipo chotero ifetikuyembekezera zimenezo.5 Ndipo wokondwa kuwona ambiri a abale athu otumikiramkati muno. Ine ndikulephera kuti ndiganizire dzina lakeapa, wamishonare, M’bale Humes ndi Mlongo Humes, kodindinu mwakhala pomwe apa, ndi ana, ndife okondwa kukhalanawo iwo, amishonare. Enawo, M’bale Pat, M’bale Daulton,ndi, oh, ambiri basi, M’bale Beeler. Ndipo ndinamuwonaM’bale Collins mphindi pang’ono zapitazo. Ndipo, oh, izozingakhale zovutirapo kuwatchula iwo onse. Koma ndifeokondwa kwambiri kukhala nanu inu mnyumba ya Ambuyeusikuuno. M’bale Neville wofunika wopambana uyu wakhalakumbuyo kwanga kuti azipemphera nane pamene ife tikhaletikuphunzitsa Mawu. Charlie, ndine wokondwa kukuwonaiwe ndi Mlongo Nellie pano usikuuno, ana. Ichi ndi…ndipo

Page 2: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

2 MAWU OLANKHULIDWA

kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde,M’bale Welch, ine basi…ndimakuyang’anayang’ana iwe, inendakuwona iwe wakhala kumbuyo uko tsopano.6 Kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhalakowopsya pang’ono, pang’ono, inu mukudziwa, zimakhala ngatiukuyenda pa ayesi wopyapyala, ife timazitcha izo. Koma ifetimangomverera kuti mwinamwake, pamene tafikapa ndipo panthawi ino, izo zingakhale zabwino kuti ndiwufikitse a—mpingoku chimene ine ndikuganiza, ku—kumvetsa kwathunthu, kwamalo ake, a chimene ife tiri mwaKhristu Yesu. Ndipo nthawizinaine ndimaganiza kuti kulalikira ndi chinthu chopambana,koma ine ndimakhulupirira nthawizina, M’bale Beeler, kutikuphunzitsa kumapita kudutsa pamenepo, iko mwabwino…makamaka kwa mpingo.

Tsopano, kulalikira kawirikawiri kumamugwira wochimwa,kumamubweretsa iye pansi pa kutsutsika ndi Mawu. Komakuphunzitsa kumamuyika munthu pamalo achimene iye ali.Ndipo ife sitingathe molondola kukhala ndi chikhulupirirompaka ife titadziwamalo athu a chimene ife tiri.7 Tsopano, ngati United States, dziko labwino ili kuno,atanditumiza ine ku Russia, ngati kazembe wa fuko lino, kuRussia, ndiye ngati iwo movomerezeka atanditumiza ine kuRussia, mphamvu zonse zimene United States ali nazo zikakhalapa nsana panga. Mawu anga akakhala chimodzimodzi basi ngatiaUnited States, ngati ine nditavomerezedwa kukhala kazembe.8 Ndiyeno ngati Mulungu watitumiza ife kudzakhalaakazembe Ake, mphamvu zonse zimene ziri Kumwamba, zonsezimene Mulungu ali, Angelo Ake onse ndi mphamvu Zake zonseziziyima kumbuyo kwa mawu athu ngati ife tiri odzodzedwamolondola, atumiki otumizidwa kwa anthu. Mulungu akuyenerakulemekeza Mawu, pakuti Iye mwaulemu analemba, kuti“Chirichonse chimene inu mudzamanga padziko lapansi,chimenecho Ine ndidzachimanga Kumwamba. Chirichonsechimene inu mudzachimasule pa dziko lapansi, chimenechoine ndidzachimasula Kumwamba. Ndipo ndikukupatsa iwemafungulo aku Ufumu.” Oh, malonjezo opambana oterowo Iyeanawapereka kwa Mpingo!9 Ndipo ine ndiri, litadutsa tsiku linalo…Ambiri a inu, inendikuganiza, munali pano mmawa uno kudzamva pamene inendimayesetsa kuti, mwanjira yanga yodzichepetsa, yophweka,ndimafotokoza ma—masomphenya amene ine ndinawawona aKumwamba.10 Ine mwanjira iliyonse sindingayesere kukaikira chirichonsechimene aliyense angandiuze ine chimene Mulungu anawauzaiwo. Ine ndikhoza kukhulupirira icho ngakhale inendisanachiwone icho mu Lemba, ine ndingafunebe kutindikhulupirire mawu a m’bale ameneyo. Ine—ine ndikhoza

Page 3: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 3

kungokhalabe ndi Baibulo, komabe ine ndikhoza kukhulupirirakutimwinamwakem’baleyo sanazimvetse izomwanjira inayake,kuti iye anangozisokoneza izo pang’ono. Ndipo komabe inendingamukhulupirire iye—iye kuti ndi m’bale wanga.11 Ndipo ngati pali chirichonse chimene chikutenthamumtimamwanga, ndipo ine ndikudalira kuti icho sichidzachoka muzaka zanga zimene zikubwerazi, kuti ine sindidzaiwala konsechimene chinachitika Lamlungu lapitali mmawa, ngati sabata.Icho chachita chinachake kwa ine chimene chasintha moyowanga. Ine—ine sindikuwopa. Ine—ine ndiribe mantha amodzia imfa. Imfa ilibe mantha konse. Ndipo iyo—iyo siingatero kwainu ngati mutangomvetsetsa. Tsopano, mwinamwake ngati…Inu mungayenere kukhala ndi chokuchitikirani kuti mudziweizo, chifukwa palibepo njira yozifotokozera izo. Inu simungathekuwapeza mawu, chifukwa iwo mulibemo mu dikishonare yaChirengezi, kapena osati mu dikishonare iliyonse, chifukwaizo ziri mu Muyaya; kunalibeko dzulo, kunalibeko mawa,zonse zinali za lero. Ndipo sizinali “ine ndikumverera bwino,”ndipo ora kuchokera pamenepo, “ine sindikumverera bwinokwambiri,” ndipo ora linalo, “ndikumverera bwino kenanso.”Zimakhala za lero nthawi zonse. Mukuona? Sizimaleka nkomwe,basi zimangokhala mtendere wa ulemelero umenewo basi,chinachake.12 Ndipo kumeneko sikungakhaleko tchimo, sikungakhalensanje, sikungakhale matenda, uko—sikungakhale chirichonsechokafika ku gombe la Kumwamba limenelo. Ndipongati ine ndingakhale ndi mwayi wonena izi, chimene,mwinamwake ine sindikhala nawo. Ngati ine sinditero, ndiyeine ndikupemphera Mulungu andikhululukire ine. Komangati ine ndingakhale nawo mwayi, ndipo iwo unali wotiMulungu anandilola ine kuti nditengedwere mmwamba kutindikawone chinachake, ine ndingaloze za Mmiyamba moyamba.Ndiyeno ine ndikukhulupirira, wina mu Baibulo, dzina lake, inendikukhulupirira anali Paulo, amene anatengedwerammwambamu Miyamba mwachitatu. Ndipo ngati munali mwa ulemelerochonchi m’Miyamba moyamba, m’Miyamba mwachitatumungakhale motani? Nzosadabwitsa iye sanayankhule za izokwa zaka fortini! Iye anati iye samadziwa kaya iye analimu thupi kapena kunja kwa thupi. Ndi mtumwi wamkuluameneyo, sikuti ndikufuna kugawana naye yake—yake—ofesiyake, kapena sikuti ndikuyesera kuti tidzipange tokha kukhalachirichonsemonga chimene iye anali, koma ine ndikhoza kunenalimodzi naye, ine sindikudziwa kaya ndinali mthupi ili kapenakunja kwa thupi. Chinthu chokhacho, izo zinali zenizeni basichimodzimodzimongammene ine ndikuyang’anira pa inu.13 Ndipo ine nthawizonse ndakhala ndikudabwa ngatindizidzadutsa ndi kuwona mtambo waung’ono ukuyandama,mzimu, ndikuti, “Apo akupita m’bale ndi mlongo, ameneyo ndi

Page 4: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

4 MAWU OLANKHULIDWA

Charlie ndi Nellie. Ameneyo ndi M’bale ndi Mlongo Spencerakupita pamenepo.” Zimenezo nthawizonse zinkandidodometsaine. Ngati maso anga adzakhala ali mmanda, akuvunda,akuwola, ngati makutu anga sali kuno kuti ndizidzamverera,ndipo ngati magazi anga onse abwerera kwawo ndipoawawumitsa iwo, ndipo iwo ali mmadzi kapena mu nthaka,ndipo ubongo wanga woganizira, makhungu a ubongo angaonse apita, ndiye ine ndingadzakhale motaninso kuposakungokhala kamzimu ndikuyandama yandama?Ndipo zimenezozinkandidandaulitsa ine. Mmene ine ndingadzakonderekudzati, “Moni, M’bale Pat, oh, wokondwa kwambirikukuwonani inu! Moni, M’bale Neville, mmene ine ndikufuniranditakuwonani inu!” Koma ine ndinaganiza, “Chabwino, ngatiine ndidzakhale ndiribe chirichonse chopenyera, kamwa iliyonseyoti ndiziyankhulira nayo, iyo yavunda, iyo ndi fumbi, inendidzatha bwanji kudzati, ‘Moni, M’bale Pat,’ ‘Moni, M’baleNeville,’ kapena zina zotero, ‘Moni, Charlie’?”14 Koma tsopano ine ndadziwa kuti uko kunali kulakwitsa.Pakuti munalembedwa mu Malemba, chimene ine ndikunenakuti sizikutsutsana, “Pakuti ngati kachisi wa dziko lapansiuyu adzaphwasuka, ife tiri naye wina amene akudikirira,”kachisi wina amene ali nawo maso, makutu, milomo,ubongo woganizira. “Ngati kachisi wa pa dziko lapansi uyuadzaphwasuka!” Iye ali nalo thupi limene ine ndikhozakumakhudza, ndikhoza kuyankhula.15 Ndipo tsopano izo zangobwera kumene kwa ine, pompano,kuti Mose anali atafa ndipo anakhala mmanda osadziwika kwazaka eyiti handiredi, ndipo Elisha anali atapita Kumwambazaka faifi handiredi mmbuyo mwake, koma pa Phiri laChiwalitsiro iwo anapezeka akuyankhulana ndi Yesu.16 Samuele atatha kufa kwa pafupifupi pakati pa zaka firiindi faifi, ndipo mfiti ya ku Endori inamuitanitsa iye, ndipo iyeanadzagwa pamaso pake, ndipo iye anati, “Iwewandinyenga ine,chifukwa iwe ndi Sauli, iwemwini.” Iye anati, “Chifukwa inendikuwona milungu!” Iye anali wachikunja, inu mwaona. “Inendikuwona milungu ikuwuka.”17 Ndipo Sauli anali asanamuwone iye apobe, ndipo iye anati,“Iye akuwonekamotani? Tamufotokozani iye kwa ine.”

Anati, “Iye ndi wochepa thupi, ndipo ali ndi chovala paphewa pake.”18 Anati, “Ameneyo ndi Samuele, mneneri, mubweretse iyekuno pamaso panga.” Ndipo ine ndikufuna kuti inu muzindikirekuti Samuele sanataye umunthu wake uliwonse. Iye analiakadali mneneri, iye anamuuza Sauli ndendende zimenezikanadzachitika tsiku lotsatira.19 Chotero, inu mukuona, imfa siimatimalizitsiratu ifekwathunthu monga mmene ife timalirira ndi kusisima ndi

Page 5: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 5

kumadandaula pa manda. Iyo imangotisinthira malo athuokhalako. Iyo imangotitengera ife malo ndi malo…Usinkhu ndichiyani? Ngati ine ndingakhale ora lina limodzi, ine ndikhozakukhala moyo kuwaposa anthu a usinkhu wa zaka sikisitiniambiri, ine ndikhoza kukhala moyo kumuposa munthu wausinkhu wa zaka faifi. Usinkhu si kanthu. Ife tinadzangoikidwakuno kwa cholinga, kuti tidzachite chinachake.20 Chabwino, tsopano, ambiri a azimayi owoneka bwino ameneakhala pano awa, ena a iwo a usinkhu wa zaka sikisitekapena sevente zakubadwa, akhoza kunena kuti, “Chabwino,ine ndachita chiyani, M’bale Branham?” Inu mwalera ana anu.Inumwachita zimenemumayenera kuti mudzachite.21 Mwinamwake Bambo wina wokalamba wakhala apa, akuti,“Chabwino, ine ndimafafaniza minda, ine ndimachita izi.Ine sindinalalikirepo.” Koma inu munangochita basi chimeneMulungu anakutumizirani inu kutimudzachite.Malo anu aliko.22 Ndikuyankhula ndi dokotala wokalamba, dzulo, mmodziwa dokotala mzanga, abwenzi, usinkhu wa zaka eyite chakutizakubadwa. Ndipo mlamu wake wamkazi ali pano mutchalitchi usikuuno, ndipo iye anakhala, wodandaula pang’onoza iye. Ndipo ine ndinapita kuti ndikamuwone iye. Ndipomwamsanga pamene ine ndinayamba kuyankhulana nayeiye, iye anachangamuka, anandiuza ine za ulendo wokasakaumene iye anali nawo zaka zambiri zapitazo kumtunda ukomu Colorado, dziko lomwelo limene ine ndimakasakako.Ali wochangamuka basi ndipo akuwala! Ndipo ine ndinati,“Dokotala, inu mwakhala mukugwira ntchito nthawi yaitalibwanji?”23 Iye anati, “Pamene iwe unkayamwa.” Ndipo mmusimwenimweni ine ndinati… “Ndipo nthawi zambiri,” iye anati,“Ine ndimagwira ntchito, kumatenga ngolo yanga, ine ndimaikazikwama za chishalo changa pa kavalo wanga. Ine ndimatengakachikwama kakang’onoko ndipo ndimayenda.”24 Ndipo ine ndinati, “Inde, kumatsikammphepetemwa gombela mtsinje, thuu koloko mmawa, muli ndi tochi yanu, kuyeserakuti mukapeze nyumba imene mwana anali ndi kupweteka kwammimba kapenamayi amene ali mu ululuwa kubala.”

“Uko nkulondola.”25 Ndipo ine ndinati, “Inu mukudziwa, adokotala, inendikukhulupirira, kudutsa mzere wolekanitsa uwu apa,pakati pa chivundi ndi chisavundi, Mulungu ali nawo maloa madokotala abwino okalamba amene anagwira ntchito mongachomwecho.”26 Misozi yaikulu inabwera mmaso mwake ndipo anayambakulira, iye anakwezera mmwamba manja ake ofooka ndipo

Page 6: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

6 MAWU OLANKHULIDWA

anati, “M’bale, ine ndikukhulupirira chomwecho.” Kutsidyalinalo,Mulungu amaweruza solo yamunthu, chimene iye ali.27 Kenako ndinamupatsa iye Lemba lokhutitsa ili. Nthawizambiri, mmayenda mminda ya mdima ya matope iyo usiku,kuyesetsa kuti mukamuthandize winawake, mwinamwakeosapezapo ndalama mukachita zimenezo, koma izo ziri bwino.Ine ndinati, “Yesu anati Mmalemba, ‘Odala ali achifundo, pakutiiwo adzalandira chifundo.’” Ndipo izo ndi zoona.28 Ndipo usikuuno ife tikufuna kuti tiwukhazikitse mpingo,mumaphunziro atatu awa, ngati Mulungu aloleza, motani ndipokodi tiziyang’ana chiyani, chimene ife tiri. Ife tiyambira pamutuwa 1 wa Bukhu la kalata ya Paulo kwa Aefeso. Ndipo ife titengamitu itatu yoyambirira mu maphunziro athu atatu otsatira,kuyesetsa kutenga mutu pa usiku, ngati ife tingathe. Usikuuno,Lachitatu, ndi Lamlungu lotsatira mmawa. Aefeso, mutu wa 1.Tsopano pamene ife tikuwerenga limodzi, ine ndikufuna kutindinene ichi, kuti Bukhu ili la Aefeso mwangwiro limafananandi YoswawaChipanganoChakale. Aefeso, Bukhu laAefeso.29 Tsopano, kumbukirani, ngati zitachitika kuti ife tachokapopang’ono, ku chiphunzitso chanu, mungotikhululukira ife ndipomupirire nafe pang’ono. Ife tisanatsegule ilo, tiyeni timufunseIye kuti atithandize ife, pamene tikuweramitsamitu yathu.30 Ambuye, ife tikuyandikira Zolembedwa Zanu zoyera ndizopatulika, chimene Izo ndi zotetezeka kwambiri kuposamiyamba yonse ndi dziko lapansi. Pakuti ife timawerenga muMawu awa, otchedwa Baibulo, kuti “Kumwamba ndi dzikolapansi zonse zidzapita, komaMawu Anga sadzalephera konse.”Ndiye, pa ora laulemu lino limene ine ndikubwera pa guwaili usikuuno, pamaso pa ogulidwa ndi Magazi Anu, achivundiodula okondedwa awa amene akhala pano usikuuno, kutengachiyembekezo chaching’ono chirichonse chimene iwo angathe,kuti agwiritsitsebe chifukwa cha Kuwala uko kumene kulinkudza. Mulole izo zikhale zokwanira kwambiri, usikuuno,kuti wokhulupirira aliyense muno awone malo ake, ndipoaliyense amene sanabwere panobe mu chiyanjano chachikuluichi, akangamire Ufumu, Ambuye, ndipo adzagogode pakhomokufikira Woyang’anirayo atatsegula chitseko. Perekani izi,Ambuye.31 Ife tikuwerenga apa pamene Baibulo ili liribe kutanthauzirakwamseri. Mulungu, musalole kuti ine wantchito Wanukapena wantchito wina aliyense adzayesere konse kudzaikakutanthauzira kwawo kwawo ku Mawu. Tiloleni ifetingowerenga Iwo ndi kuwakhulupirira Iwo, mmene Iwoanalembedwera. Ndipo makamaka ife azibusa a nkhosa, ifeabusa amene tsiku lina tidzakasonkhana uko mu Dziko laulemelero lija ndi nkhosa zapang’ono, ndipo tidzakaima muKukhalapo kwa Ambuye Yesu ndipo tidzawuwona m’badwo

Page 7: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 7

umenewo ukutulukira, wa Paulo, ndi wa Petro, ndi wa Luka,ndi Marko, ndi Mateyu, ndi onse awo, ndipo tidzawawona iwoakuweruzidwa kumeneko ndi magulu awo. Mulungu, perekanikuti ine ndidzathe kudzaika zikho teni millioni pa mapaziAnu pamene ine modzichepetsa ndizidzakwawira chokwerandi kudzaika manja anga pa mapazi Anu ofunika, ndikuti,“Ambuye, iwo ndi Anu.”32 O Mulungu, tidzadzeni ife mwatsopano ndi Mzimu Wanu,ndipo ndi chikondi Chanu ndi ubwino Wanu. Ndipo mulole ife,monga wandakatulo anafotokozera mu nyimbo zaka zambirizapitazo, “Wokondedwa Mwanawankhosa wakufa, MagaziAnu ofunikira sadzataya mphamvu yake, mpaka Mpingowonse wowomboledwa wa Mulungu udzapulumutsidwe kutiusadzachimwenso. Ndipo kuyambira nthawi imeneyo, mwachikhulupiriro, ine ndinawona mtsinje uja umene mabala Anuosefukira amapereka; chikondi chowombola chakhala chirinkhani yanga, ndipo idzakhala mpaka ine ndidzafe. Kenakomu nyimbo yochirimika, yokoma,” iye akupitirira kumati,“Ine ndidzaimba mphamvu Yanu yopulumutsa; pamene lirimelosauka losayankhula bwino ili, lachibwibwi lidzagone chetemmanda.” Zikadzatero, manda sadzagwira imfa iliyonse ya anaAnu. Iyo ndi malo opumulirako chabe, kapena malo obisalako,kumene chivundi ichi chiti chidzakavale chisavundi.33 Mulole ife usikuuno tiziwone izi, Ambuye, pambalambanda,monga izo zinaperekedwera kwa ife mu Mawu. Tipatseni ifekumvetsa. Ndipo mukatiike ife, Ambuye, pa malo athu antchito, kuti ife tikakhoze kutumikira mokhulupirika mpakaInu mudzabwere. Ife tikupempha izi mu Dzina la Yesu, ndichifukwa cha Iye. Ameni.34 Tsopano, Bukhu la Aefeso, monga mmene inendimangonenera, ine…mwa kuganiza kwanga, ndi limodzila Mabukhu opambana kwambiri a Chipangano Chatsopano.Ilo limakatisiya ife, kumene Chikalvini chimakayenda panthambi imodzi, ndipo Chiarminia chimakayenda pa nthambiinayo, koma Bukhu la Aefeso limabweretsa izo pamodzi ndikudzawuika Mpingo pamalo ake.35 Tsopano, ine ndazifanizitsa izo ndi Yoswa. Ngati inumungazindikire, Israeli anatulutsidwa kuchokera ku Igupto,ndipo panali magawo atatu a ulendo wawo. Gawo limodzi, linalikuchoka ku Igupto. Gawo lotsatira, linali mchipululu. Ndipogawo lotsatira, linali Kenani.36 Tsopano, Kenani samaimira m’badwo wa Zakachikwi. Iyeamangoimira m’badwo wa mgonjetsi, kam’badwo kogonjetsa,chifukwamuKenani iwo amapha ndi kuwotcha ndipo amalandamizinda. Ndipo simudzakhala imfamuZakachikwi.37 Koma chinthu china chimene iye amachita, iyeamabweretsa kulungamitsidwa mwa chikhulupiriro, iwo atatha

Page 8: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

8 MAWU OLANKHULIDWA

kumukhulupirira Mose ndi kuchoka ku Igupto. Kuyeretsedwa,kumatsatira pansi pa Lawi la Moto ndi chitetezero chamwanawankhosa wa nsembe mu chipululu. Ndipo kenakonkudzalowamdziko limene linali litalonjezedwa.38 Tsopano, kodi dziko lolonjezedwa kwa wokhulupirira waChipangano Chatsopano ndi liti? Lonjezolo ndi Mzimu Woyera.“Pakuti kudzachitika mmasiku otsiriza,” Yoweri 2:28, “kuti inendidzatsanulira Mzimu Wanga pa thupi lonse. Ana anu aamunandi aakazi adzanenera. Ndipo pa antchito Anga ndi adzakaziAnga ine ndidzatsanulira Mzimu Wanga, ndipo iwo adzanenera.Ine ndidzawonetsa zodabwitsa mmiyamba mmwamba. Ndimdziko lapansi, malawi a moto, ndi utsi, ndi mame.” NdipoPetro anati, pa Tsiku la Pentekoste, atatenga phunziro lake ndiponkumalalikira, “Lapani, aliyense wa inu, ndipo mubatizidwemu Dzina la Yesu Khristu kuloza ku chikhululukiro,” kuchotsa,kukhululuka, kuchotsa zolakwa zammbuyo zonse.39 Kodi inu munazindikira, Yoswa, iwo asanawoloke Yordani,Yoswa anati, “Mupite pakati pa msasawo ndipo mukachapezovala zanu ndipo mukadziyeretse mmodzi aliyense wa inu,ndipo musakalole mwamuna aliyense akagone ndi mkaziwake, pakuti mmasiku atatu inu muwona Ulemelero waMulungu.” Mukuona? Iyo ndi—iyo ndi ndondomeko yokonzekerakukalandira lonjezolo. Tsopano, lonjezo kwa Israeli, linali,Mulungu anamupatsa Abrahamu lonjezo la dziko, la Palestina,ndipo ilo linali loti lidzakhale cholowa chawo kwa nthawizonse.Ndipo iwo anali woti azikhalamdziko ili nthawizonse.40 Tsopano, iwo anabwera mmagawo atatu, akubwera kudziko lolonjezedwa ili. Tsopano penyani, izo zikufanizidwamwangwiro mu Chipangano Chatsopano.41 Tsopano izi, monga ine ndanenera, zimatsutsana ndikuganiza kwina kwa inu. Ena a inu anthu ofunikira achiNazarene, Church of God, ndi ena otero, musalole kuti izizikupwetekeni, komamungowona izomwatcheru ndipomuwonezoimira zake. Mupenye ndipo muwone ngati malo aliwonsesakugunda mwangwiro basi.42 Kunali magawo atatu a ulendowo, ndipo alipo magawoatatu a ulendo uno. Pakuti, ife timalungamitsidwa mwachikhulupiriro, kukhulupirira paAmbuye YesuKhristu, kulisiyadziko la Igupto, kutulukamo. Ndipo kenako nkudzayeretsedwakudzera mu kupereka kwa Magazi Ake, kusambitsidwa kumachimo athu, ndi kudzakhala amwendamnjira ndi alendo,kumadzinenera kuti tikufunafuna dziko, mzinda umeneukubwera, kapena lonjezo.43 Chomwechonso anatero Israeli mu chipululu, apaulendo,opandamalo opumulirako, akuyenda usiku ndi usiku, akutsatiraLawi la Moto, koma potsiriza anadzafika ku dziko lolonjezedwakumene iwo anadzakhazikikako.

Page 9: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 9

44 Kumeneko ndi kumene wokhulupirira amadzafikako.Poyamba iye amabwera pozizindikira kuti iyeyo ndi wochimwa;kenako iye amadzalekanitsidwa ndi madzi, kusambitsidwa kwamadzi, mwa Magazi, ndipo…kapena kusambitsidwa ndi madzimwa Mawu, kani, kukhulupirira pa Ambuye Yesu Khristu.Ndiye, polungamitsidwa mwa chikhulupiriro, iye amadzakhalawotenga nawo, ndipo amakhala pa mtendere ndi Mulungu,kudzera mwa Khristu, kubatizidwa kulowa mu Dzina la YesuKhristu, kukamulowetsa iye mu ulendo. Inu mukumvetsazimenezo? Kukalowa mu ulendo! Kenako iye amadzakhalawapaulendo ndi mwendamnjira. Iye amakhala ali pa ulendowakewopita ku chiyani? Lonjezo limeneMulungu anapanga.

45 Israeli anali asanalandirebe lonjezo, koma iwo analiali pa ulendo wawo. Ndipo musananyamukepo…Chondetamvetserani. Pamenepo ndi pamene inu, a Nazarene ndi aPilgrim Holiness, ndi ena otero, munalepherera. Chifukwa,Israeli, pamene iwo anadzafika pamalo amenewo, a Kadesh-Barnea, pamene azondi anapita uko ndikuti, “Dzikolo ndilabwino.” Koma ena a iwo anabwerera ndikuti, “Ife sitingathekulitenga ilo, chifukwa mizindayo ili ndi malinga, ndi zinazotero.” Koma Yoswa ndi Kalebu anaimirira, ndipo anati, “Ifendi oposa kuthekera kulitenga ilo!” Chifukwa mfundo zawozinali zitalembedwa kale ndi kusainidwa, iwo ankakhulupiriramu ntchito ziwiri za chisomo, kulungamitsidwa ndikuyeretsedwa, ndipo sanathe kusunthira mtsogolo mulimonse.Ndipo, mvetserani, kam’badwo konseko kanakathera muchipululu. Koma awiri amene anakalowamdziko lolonjezedwalondipo anabweretsako umboni wakuti ilo ndi dziko labwino,“ndipo ife tinali othekera kulitenga ilo, chifukwa ilo linalilonjezo la Mulungu.” Ndiye mmalo moti anthuwo azipitirirapatsogolo, kukalandira Mzimu Woyera, kukayankhula ndimalirime, kukalandira mphamvu ya Mulungu, ubatizo waMzimu Woyera, zizindikiro, zodabwitsa, zozizwitsa, iwoanamverera kuti izo zikhoza kusokoneza mwambo wawo wachiphunzitso. Ndipo chinachitika nchiyani kwa izo? Anaferamdzikolo! Uko nkulondola!

46 Koma okhulupirira, onga ngati Kalebu ndi Yoswa, ameneamapitirira kupita ku lonjezo, iwo anasamukira mpaka kudzikolo, ndipo anakalitenga dzikolo, ndipo anakakhazikikamdzikolo, ngati cholowa. Ndipo ife sitimaimira konse pakulungamitsidwa, kuyeretsedwa. Tiyeni tipitirire mpaka kuubatizo wa Mzimu Woyera. Tiyeni tisaimire pa kukhulupiriraAmbuye Yesu, kungobatizidwa. Tiyeni tisaimire chifukwa Iyeanatiyeretsa ife ku moyo wa tchimo. Koma tsopano ifetikakamire mpaka tikafike ku malowo, ku lonjezo la ubatizowa Mzimu Woyera. Pakuti Petro anati, pa Tsiku la Pentekoste,“Pakuti lonjezo liri kwa inu, ndi kwa ana anu, ndi kwa iwo

Page 10: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

10 MAWU OLANKHULIDWA

amene ali kutali, ngakhale onse amene Ambuye Mulungu wathuadzawaitana.”47 Chotero, Aefeso apa akutiika ife monga Yoswa, kutiikapamalo. Inu mukuzindikira, Yoswa, atawolokera ku dzikolo,ndipo nakatenga dzikolo, kenako iye analigawaniza dzikolo,“Efremu apa, Manasse apa, ndipo uyu apa, Gadi apa, Benjaminapa.” Iye analigawa dzikolo.48 Ndipo zindikirani! Oh, ichi chikutenthetsa mitima yathu!Aliyense wa amayi achi Hebri amenewo, akubereka anaamenewo, iye amawayankhula malo enieniwo, mu ululuwake wakubala, kumene iwo akanati adzaikidwe mu dzikololonjezedwalo. Oh, ndi phunziro lalikuru! Ngati ife tingapitemmenemo mwatsatanetsatane, zimene zingatenge maorapambuyo pa maora. Tsikulina ife tikadzakonza tchalitchichathu, ine ndikufuna kuti ndidzangobwera ndi kudzatengamwezi wathunthu kapena iwiri, basi kudzangokhala mmenemo.Penyani pamene iwo, aliyense wa amayi amenewo, pamene iyeankaitana, “Efremu,” pamene iye anali mu kubereka, anamuikaiye pamalo amene mapazi ake anali ataponda mmafuta. Basindendende aliyensewa iwo paliponse pamene iwo anali!49 Ndipo Yoswa, asakudziwa izi, koma mwa kudzoza,motsogozedwa ndi Mzimu Woyera, atatha kukalowa mdzikololonjezedwalo, anamupatsa munthu aliyense lonjezo lake,ndendende chimene Mzimu Woyera unalonjeza kudzera mukubadwa kumbuyo uko.50 Mmene Mulungu wawaikira ena mu mpingo, kudzera muululu wakubala! Oh, iwo amakhala opambana nthawizina.Pamene mpingo ukubuula pansi pa kuzunzika kwa dzikolakunja, kukhulupirira pa Ambuye Yesu, kuti lonjezo la MzimuWoyera ndi lenileni basi kwa ife monga ilo linali kwa Pentekoste,mmene iwo ankabuulira ndi kulira pansi pa ululu wakubala!Koma pamene iwo abadwa, ndipo nkubadwira pa malo awomu Ufumu wa Mulungu, ndiye Mzimu Woyera umawaika mumpingo, ena atumwi, ena aneneri, ena aphunzitsi, ena abusa,ena avangeri. Ndiye Iye amapereka mmenemo, kuyankhulandi malirime, kutanthauzira kwa malirime, chidziwitso, nzeru,mphatso zamachiritso, mitundu yonse ya zozizwitsa.51 Kumene kuli mpingo…Tsopano ichi ndi cholinga changachochitira izi. Mpingo nthawizonse ukumayesetsa kutengangodya ya winawake. Koma musamachite zimenezo. Inusimungalime chimanga pa ngodya ya Efremu, ngati inu muliManasse. Inu mukuyenera kutenga malo anu mwa Khristu,kuwatenga iwo pamalo ake. Oh, izo zimazama ndi kukhuthalapamene ife tilowa umu, mmene Mulungu amamuikira winamu mpingo kuti aziyankhula mmalirime, wina…Tsopano,ife taphunzitsidwa nthawi zambiri, “ife tonse tikuyenerakuyankhula ndi malirime.” Zimenezo nzolakwika. “Ife tonse

Page 11: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 11

tikuyenera kuchita izi.” Ayi, ife sititero. Iwo onse sankachitachinthu chimodzi. Aliyense anali…52 Aliyense, dzikolo linaperekedwa ndi kugawidwa mwakudzoza. Ndipo, aliyense, ine ndikhoza kutenga Malemba ndikuwonetsa izo kwa inu ndendende, kuti iye anakawayika iwopa malo amene iwo ankayenera kukhalapo, pamalo awo, mmenemafuko awiri athekawo anali woti akakhale kutsidya kwamtsinje, mmene amayi awo ankalirira zimenezo mu kubadwakwawo, ndimmenemalo aliwonse ankayenera kukhalira.53 Ndipo tsopano inu mutatha kulowa, zimenezosizikutanthauza kuti inu simumakhala ndi nkhondo. Inumukuyenera kuti muzimenyerabe inchi iliyonse ya maloamene mwaimapowo. Chotero, mwaona, Kenani sankaimiraKumwamba kwakukulu, chifukwa kumakhala nkhondo ndimavuto ndi kuphana ndi kumenyana, ndi zina zotero. Koma iyeankaimira ichi, kuti kumayenera kukhala kuyenda kwangwiro.54 Pamenepo ndi pamene mpingo ukulephera lero, pa kuyendakumeneko. Kodi inu mukudziwa kuti ngakhale khalidwe lanulomwe likhoza kumugwetsa winawake kuti asachiritsidwe?Kupanda khalidwe kwanu, kwa machimo osalapa a inuokhulupirira, kukhoza kuwupangitsa mpingo uwu kulepheramoipa. Ndipo pa Tsiku la Chiweruzo inu mudzakayankhiragawo lirilonse la izo. Oh, inu mukuti, “Tsopano, dikiraniminiti, M’bale Branham.” Chabwino, chimenecho ndi Choonadi.Taganizani za izo!55 Yoswa, iye atatha kuwolokera mdzikolo, Mulunguanamupatsa iye lonjezo limene…Tangoganizani, kumenyankhondo yonseyo opanda kutaya munthu mmodzi, opandangakhale kukandika nkomwe, opanda ngakhale kukhala ndinamwino, kapena chithandizo choyambirira kapena bandeji.Ameni.Mulungu anati, “Dzikolo ndi lanu, pitanimukamenyere.”Taganizani, kumenya nkhondo, ndipo opanda kukhala ndi a RedCross nkomwe pafupi, palibe aliyense amene ati akavulale!56 Ndipo iwo anawapha a Amori ndi a Hitti, koma kunalibekommodzi amene anavulala pakati pa aliyense wa iwo mpakatchimo litadzabwera mu msasa. Ndipo pamene Akanianadzatenga chovala cha wachi Babeloni uja ndi chikutecha golide chija, ndi kukazibisa izo pansi pa msasa wake,atatero tsiku lotsatira iwo anataya amuna sikisitini. Yoswaanati, “Imani! Imani! Dikirani miniti, pali chinachake chimenechalakwika! Chinachake chalakwika apa. Ife tiitanitsakusala kwa masiku seveni. Mulungu anatipangira ife lonjezo,‘Sipadzakhala chirichonse chiti chidzativulaze ife.’ Adani athuadzagwera pa mapazi athu. Ndipo pali chinachake chalakwikaapa. Chinachake chalakwika penapake, chifukwa ife tiri ndiamuna sikisitini omwe afa agona apa. Iwo ndi abale achi Israeli,ndipo iwo afa.”

Page 12: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

12 MAWU OLANKHULIDWA

57 Nchifukwa chiyani iwo anafa, munthu wosalakwa?Chifukwa munthu mmodzi anachoka pa mzere. Inu mukuwonachifukwa chimene izi zikuyenera kuphunzitsidwa? Mpingouzifola, uzifola ndi Mawu a Mulungu, uzifola ndi Mulungundipo uzifola ndi wina ndi mzake, kumayenda mwangwiromowongoka, moganiza bwino, pamaso pa anthu onse,kumawopa Mulungu. Chifukwa munthu mmodzi ataba chovala,ndipo atachita chinachake chimene iye samayenera kuti achite,zinatenga moyo wa anthu sikisitini! Ine ndikuganiza analisikisitini, mwinamwake ochulukirapo. Ine ndikukhulupiriraanali amuna sikisitini amene anafa.58 Yoswa anaitanitsa, anati, “Pali chinachake chalakwika!Mulungu anapanga lonjezo, ndipo chinachake chalakwika.”59 Pamene ife tibweretsa odwala pamaso pathu, ndipo iwonkulephera kuti achiritsidwe, ife timayenera kuti tiziitanitsakusala kwaulemu, tiziitanitsa msonkhano. Chinachakechalakwika penapake. Mulungu anapanga lonjezo, Mulunguakuyenera kukakamira ku lonjezo limenelo, ndipo Iye adzachitaizo.60 Ndipo iye anaitanitsa kusala. Ndipo iwo anadzapeza kuti,iwo anapanga maere. Ndipo Akani anavomereza izo. Ndipo iwoanamupha Akani, banja ndi onse, ndipo anawotcha maphulusaawo, ndipo analisiya ilo kumeneko ngati chikumbutso.Ndipo Yoswa anapitirira kudutsa mu nkhondoyo, kumatengachirichonse, opanda kukandika kapena bala. Ndi zimenezotu.61 Tsiku lina iye ankafuna kanthawi pang’ono, nthawiyowonjezera. Dzuwa linali likukalowa, amunawo samathakumenya bwino bwino pa nthawi ya usiku. Yoswa, wankhondowamkulu uja, wodzozedwa wa Mulungu, woikidwa pamalomu dzikolo, monga Aefeso ku Mpingo watsopano, kutenga,anatenga, anatenga dzikolo, analilanda ilo. Iye ankafunakanthawi, chotero iye anati, “Dzuwa, ima njii!” Ndipo ilolinaima njii kwa pafupifupi maora thwelofu, mpaka iyeatalitenga dzikolo. Mukuona?62 Tsopano Bukhu la Aefeso limatiika ife pamalo athu mwaKhristu, chimene iwo anali mu Dziko Loyera. Ife sitikuikidwamu Dziko Loyera, koma mwa Mzimu Woyera! Tsopano tiyeni ifetingowerengaMawu, tiwonemmenempingo uliri wangwiro.

Paulo, mtumwi wa Yesu Khristu mwa chifuniro chaMulungu,…

63 Oh, ine ndikuzikonda zimenezo! Mulungu anamupanga iyekukhala mtumwi. Panalibe ma eledara amene anadzaika manjapa iye, panalibe mabishopu amene anamutumiza iye kulikonse,koma Mulungu anamuitana iye ndipo anamupanga iye kukhalamtumwi.

Page 13: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 13

Paulo, mtumwi wa Yesu Khristu mwa chifuniro chaMulungu, kwa oyera (iwo oyeretsedwawo) amene ali kuEfeso, ndi kwa okhulupirika mwa Yesu Khristu:

64 Penyani mmene iye akuyankhulira izi. Izi si za kwaosakhulupirira. Izi ndi za kwa mpingo. Izo zikuitanidwira kwaoitanidwa atuluke awo, oyeretsedwa ndi oitanidwa amene alimwa Khristu Yesu.

65 Tsopano, ngati inu mukufuna kuti mudziwe mmene ifetimalowera mwa Khristu Yesu, ngati inu mungatsegule kuAkorinto Woyamba 12, iye amati, “Pakuti mwa Mzimu umodziife tonse timabatizidwa kulowa mu Thupi limodzi.” Motani?Pobatizidwa motani? Mzimu Woyera. Osati mwa ubatizowa mmadzi, inu anthu a Church of Christ, koma mwachilembo chachikulu M-z-i-m-u, mwa Mzimu umodzi. Osatimwa kugwirana chanza kumodzi, mwa kalata imodzi, osatimwa kukonkha kumodzi. Koma mwa Mzimu umodzi ife tonsetimabatizidwa kulowa mu Thupi limodzi, cholowa chathu,dziko limene Mulungu anatipatsa ife kuti tizikhalamo, MzimuWoyera. Chimodzimodzi basi monga Iye anamperekera Kenanikwa Ayuda, Iye watipatsa ife Mzimu Woyera. Mwa Mzimuumodzi ife tonse timabatizidwa kukalowamu Thupi limodzi. Inumukumvetsa zimenezo?

66 Tsopano, iye akuyankhula kwa Akenani auzimu, Israeli,Israeli wauzimu amene watenga dziko. Oh, kodi sindinuokondwa kuti mwachoka ku gariki waku Igupto? Kodi sindinuokondwa kuti mwatuluka mchipululu? Ndipo, kumbukirani,iwo ankayenera kuti azidya manna, chakudya cha Angelochochokera Kumwamba, mpaka iwo atawoloka kukalowamdzikolo. Ndipo pamene iwo anadzawoloka kukalowamdzikolo, manna anasiya kugwa. Iwo anali atakhwimakwathunthu nthawi imeneyo, ndipo iwo amadya chimangachakale cha mdzikolo. Tsopano, tsopano pakuti sindinumakanda panonso, tsopano pakuti inu simukukhumbansomkaka woyenera wa Uthenga, kuti inu simukusowa kutimuzichita kuleledwa, ndi kusisitidwa, ndi kumachitakunyengereredwa kuti mubwere ku tchalitchi, tsopano pakutindinu Akhristu okhwima kwathunthu, ndinu okonzeka kudyachakudya cholimba tsopano. Ndinu okonzeka kuti mubwereku chinachake, iye anatero. Ndinu okonzeka kuti mumvetsechinachake chimene chiri chakuya ndi chodula. Oh, ife tilowamu zimenezo molunjika. Ndipo, oh, izo zakhala zobisidwakuyambira pa maziko a dziko lapansi. Iye anati, “Tsopanopakuti inu mwabwera mu izi, ine ndikuyankhula izi kwa inu.”Osati kwa iwo amene angochoka kumene Igupto, osati kwaiwo amene akadali pa ulendo, koma kwa iwo amene ali mdzikololonjezedwa, amene alandira lonjezo.

Page 14: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

14 MAWU OLANKHULIDWA

67 Ndi angati amene analandira lonjezo la Mzimu Woyera? Oh,kodi sindinu okondwa kuti muli mdziko pano tsopano, mukudyachimanga chakale, mukudya zinthu zolimba za Mulungundipo muli nako kumvetsa komveka. Anu—maganizo anu onseauzimu ndi osasokonezeka. Inu mukudziwa ndendende kutiIye ndi ndani. Inu mukudziwa ndendende chimene Iye ali. Inumukudziwa ndendende kumene inu mukupita. Inu mukudziwandendende zonse za Izo. Inu mukudziwa mwa Amene inumwamukhulupirira ndipo wokhutitsidwa kuti Iye ndi wokhozakusunga chimene inu mwapereka kwa Iye mu tsikuli. Oh, ndiameneyotu, ameneyo ndi yemwe Paulo akuyankhulana nayetsopano. Mvetserani mwatcheru. Tsopano penyani.

…okhulupirika mwa Khristu Yesu:68 Tsopano, ndikufuna mpingo ubwereze zimenezo. Ifetimalowa chotani mwa Khristu? Pojowina mpingo? Ayi. Poikadzina lathu pa bukhu? Ayi. Pobatizidwa mwakumiza? Ayi.Timalowa chotani mwaKhristu? MwaMzimuWoyera umodzi ifetonse timabatizidwa kukalowamu lonjezo limodzi, Thupi, ndipotimakhala otenga nawo a zonse zimene ziri za mdzikolo. Ameni!Oh, ine—ine ndikuzikonda zimenezo. Ngati ine ndikanakhalakuti sindinasase mawu, ine ndikanafuula. Mai, pamene inendidzafike mu dziko ili, ilo ndi langa. Ine ndiri kwathu tsopano;ine ndiri mu Kenani. Ndine womvera kwa chirichonse chimeneMulungu akufuna kuti andigwiritseko ntchito. Ine ndikuyendammalo oyera, mwana wa Mfumu, yense wovekedwa mwinjirondipo wokonzeka. Ine ndatuluka ku Igupto, ndabwera kudutsamdziko lolonjezedwa, ndapirira mayesero, ndadutsa ku Yordanindipo ndafika ku lonjezo lodala ili. Oh, ine ndinazipeza motaniizo? Mwa Mzimu umodzi. Mwanjira yomweyo imene Pauloanawupezera Iwo, unachita pa ine mwanjira yomweyo imeneIwo unachitira pa iye, mwanjira yomweyo imene Iwo unachitirapa inu. Mwa Mzimu umodzi ife tonse timabatizidwa. Osatikukonkhedwa, kukonkha pang’ono chabe kwa Iwo, kumvererabwino kwambiri; koma kumizidwa pansi! Zonse kupangitsidwakuti zisambire pansi, muMzimuWoyera. Ndiro lonjezo.69 Aefeso wathu, Yoswa wathu, amene ali Mzimu Woyera,Yoswa amatanthauza “Yesu, Mpulumutsi.” Yoswa kutanthauzaMzimu Woyera kuimira izo mwauzimu monga izo zinali muthupi, kuti Iye ndi Wankhondo wamkulu wathu. Iye ndiMtsogoleri wathu wamkulu. Chimodzimodzi monga Mulunguanali ndi Yoswa, chomwechonso Mulungu (mwa MzimuWoyera) akutiyendetsa ife. Ndipo pamene tchimo libwera mumsasa, Mzimu Woyera umafuna kuimikira, “Chalakwika ndichiyani mu mpingo uno? Chinachake chalakwika.” Oh, inusimukuwona mmene ife takhalira ndi ana aamuna ambiria Kish tsopano? A Saulo ochuluka akubwera kuchokeraku maseminare ndi masukulu a zaumulungu ndi kumapitakunja ndi kumakaphunzitsa zinthu zopotozedwa izi, monga

Page 15: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 15

Baibulo linanena kuti iwo akanadzachita. “Mowoneka,opanda Chikhulupiriro, kudzilekanitsa okha kwa inu, opandachiyanjano ndi inu, ndi zina zotero, okhala nawo mawonekedweaumulungu ndipo nkumakana Mphamvu yake, kwa iwochokaniko.” Iwo sakudziwa kumene iwo anachokera, iwosangapereke chifukwa chirichonse.70 Ine ndikunena izi kuchokera kwa M’bale Booth Clibborn,mzanga wa ine, ngati pali chirichonse chimene chiri…chapathengo chosalengedwa ndi mulungu, chirichonse mdziko,ndi mphongolo. Mphongolo ndi wotsikitsitsa wa zinthu zonse.Iye ndi a…iye—iye samadziwa chimene iye ali. Iye sangathekudzibereka yekha nkomwe. Mphongolo sangakweranitsidwendi mphongolo imzake ndi kudzakhalanso mphongolo. Iyewatha. Iye samadziwa kumene abambo ake amachokerako,komanso samawadziwa amayi ake, pakuti iye ndi wamng’ono—bulu wamng’ono ndi kavalo wamba. Mulungu sanapangekonse zimenezo. Musamaziike zoterozo pa Mulungu. Mulungusanapange konse zimenezo. Mulungu anati, “Chirichonsechidzabala za mtundu wake.” Inde, bwana. Koma mphongolondi—a…bambo ake anali bulu ndipo mayi ake anali kavalowamba, chotero iye samadziwa kuti iye ndi wandani. Iye—iye—iye ndi kavalo woyesetsa kuti akhale mphongolo, kapenamphongolo…kapena—kapena iye ndi kavalo woyesetsa kutiakhale bulu, bulu akuyesetsa kuti akhala kavalo. Iye samadziwakuti iye ndi wakuti. Ndipo iye ndi chinthu choumamutu chimenechiripo mdziko. Inu simungaike konse chidaliro chirichonsepa iye.71 Ndipo umo ndi mmene anthu ambiri aliri mu mpingo.Iwo samadziwa kuti bambo wawo ndi ndani, iwo samadziwakuti mayi wawo ndi ndani. Chinthu chokhacho chimeneiwo amachidziwa, mwinamwake iwowo ndi a Presbateria,Methodisti, Baptisti, kapena Pentekoste, kapena chinachake.Iwo samadziwa kumene iwo anachokera. Ndipo buluwokalamba, inu mukhoza kumukuwira iye mmene inumungafunire kumukuwa iye, ndipo iye angaime pamenepondi kuimitsa makutu aakulu awo, ndi kumangoyang’ana.Iwe ukhoza kulalikira kwa iwo utali wa usiku wonse, ndipoakamachokapo osadziwa konse kalikonse kuposa mmeneamadziwira pamene amadzalowa. Tsopano, izo ndi kulondolabasi. Ine sindikutanthauza kuti ndikhale wamwano, koma inendikufuna kuti ndikuuzeni inu Choonadi.72 Komapali chinthu chimodzi chimene iwo amakhoza kuchita,iwo ndi ogwira bwino ntchito. Oh, iwo amangogwira, kugwira,kugwira, kugwira. Zimenezo zimandiika ine mmalingaliroa gulu la Achiarminia ili amene nthawizonse amayesetsakugwirira ntchito ulendo wawo wopita Kumwamba. Ukonkulondola, mphongolo. Oh, a Ladies Aid Society, ndi mgonerowa nkhuku, ngati malipiro, a mlaliki. “Ndipo tikhale ndi zovina

Page 16: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

16 MAWU OLANKHULIDWA

izi, ndi zosangalala izi.” Iyo imangokhala ntchito, ntchito,ntchito, ntchito, ntchito, ntchito, ntchito. Ndipo, iwo, kodi iwoakugwirira ntchito chiyani?73 Ukawafunsa iwo, “Kodi inu munalandira Mzimu Woyerakuyambira pamene inu munakhulupirira?”74 Iwo amaimitsa makutu awo, ndipo iwo samadziwa kutiiwo ndi akuti, “Kodi inu mukutanthauza chiyani? Ndikutikumene kunachitika zonse izi? Inu mukutanthauza chiyani,Mzimu Woyera? Ine sindinamvepo chirichonse cha Iwo. Oh,iwe ukuyenera kukhala mtundu winawake wa otengeka.”Mwaona, iwo samadziwa kuti bambo anali ndani, kapenaamayi anali ndani, aponso. Ndipo iwe umachita kuwamenyaiwo pa chirichonse chimene iwe ukuchita, kumenya apa ndikudzamenya apo, ndi kumenya apa ndi kudzamenya apo. Ukonkulondola, mphongolo yakale.75 Koma, ine ndikukuuzani inu, inu simumasowakuchita zimenezo ndi kavalo wa mtundu weniweni.Mukangomukwapula iye kamodzi chikwapu, ndipo m’bale,iye wapita. Iye amadziwa chimene iye akuchita. Oh, zimakhalazabwino bwanji kukwera wa mtundu weniweniyo! Zimakhalazabwino bwanji kunena kuti, “Tiyeko, mnyamata.” Oh, mzanga,zingakhale bwino kuti ugwiritsitse, angachiponyere mmwambachishalocho.76 Umo ndi mmene zimakhalira ndi Akhristu enieni. Aleluya!“Landirani inu Mzimu Woyera. Lapani, aliyense wa inu,ndipo mubatizidwe mu Dzina la Yesu Khristu, kuloza kuchikhululukiro cha machimo anu.” Amapita, basi mwamsangamonga mmene iwo angathere kupita ku madzi, iwo amapita.Iwo sangapume usana ndi usiku mpaka iwo atalandira MzimuWoyera. Bwanji? Inu mukudziwa, Mkhristu amadziwa kutibambo ake anali ndani. Mwaona, zimatengera awiri kutipakhale kubadwa.Uko nkulondola, bambo ndimayi.Mphongolosiimadziwa kuti bambo anali ndani, kapena amayi analindani. Koma ife timadziwa kuti Bambo ndi Mayi anali ndani,pakuti ife tinabadwa mwa Mawu olembedwa a Mulungu,tinatsimikiziridwa ndi Mzimu. Petro anatero, pa Tsiku laPentekoste, “Ngati inu mulapa ndi kubatizidwa, mmodzialiyense wa inu, mu Dzina la Yesu Khristu, ku chikhululukirocha machimo anu, inu mudzalandira mphatso ya MzimuWoyera.”77 Ndipo, m’bale, Mkhristu weniweni wobadwa mwatsopano,(oh, mai) mzimu wake, mwamsanga iye akalandira Mawu,iye amalandira Mzimu Woyera. Mfunseni iye chinachakenthawi imeneyo! Iye amadziwa pamene iye wayima. “Kodi inumumakhulupirira mumachiritso Auzimu?”

“Ameni!”“Kodi inumumakhulupiriramuKudzaKwachiwiri?”

Page 17: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 17

“Ameni!”78 Ifunseni mphongolo zimenezo. Chipembedzo champhongolo, “Uh, ine sindikudziwa. Dokotala Jones ananenanthawi ina…”Huh! Pamenepo, akumutsatira Saulo. Mukuona?“Oh, iwo sakudziwa. Chabwino, ine ndikukuuzani inu, mpingowanga siuli wotsimikiza za Izo.”79 Oh, m’bale, koma mwamuna wobadwa mwatsopano ndimkazi amakhala otsimikiza basi za kudza kwa Ambuye Yesu,iwo amakhala otsimikiza basi kuti analandira Mzimu Woyerapakuti MzimuWoyera ulipo woti uperekedwe.80 Tsopano, Yesu anati…Mkazi pa chitsime, “Ifetimapembedza mu phiri ili, ndipo Ayuda amapembedza kuYerusalemu.”81 Iye anati, “Mkazi, mvera Mawu Anga! Ora likubwera,ndipo tsopano liripo, pamene Atate akufuna iwo ameneazimupembedza Iye muMzimu ndi Choonadi.”82 Mawu Anu ali Choonadi. Ndipo munthu aliyense ameneadzawerenga Baibulo ndi kukhulupirira Mawu aliwonse ameneBaibulo likunena, ndi kutsatira malangizo Ake, ndi kulandiraMzimu Woyera womwewo umene iwo analandira, mwanjirayomweyo imene iwo analandilira Iwo, zotsatira zomwezo zimeneiwo analandilira Iwo, mphamvu yomweyo imene iwo anaipezapamene analandira Iwo, iye amadziwa yemwe Bambo wakendi Amayi anali. Iye amadziwa kuti iye anasambitsidwaMmagazi a Yesu Khristu, anabadwa mwa Mzimu, anadzazidwandi kudzodza kwa Mulungu. Iye amadziwa pamene iyeakuima. Ndithudi! Iye ali mu Kenani. Iye amadziwa kumeneiye anachokera. Umo ndi mmene zimakhalira ndi Mkhristuweniweni. Mukamufunsa iye, “Kodi iwe unalandira MzimuWoyera chikhulupirireni?”

“Ameni, m’bale!”83 Nditaima tsiku lina pafupi ndi woyera wakale, usinkhu wazaka nainte-thuu, akuyankhulana ndi m’busa wake wa usinkhuwa zaka eyite, ine ndinati, “Agogo aakazi?”

Wowala basi monga mmene iye akanakhalira, iye anati,“Inde, mwana wanga.”84 Ine ndinati, “Zatenga nthawi yaitali bwanji kuyambirapamene munalandira MzimuWoyera?”

Iye ndinati, “Ulemelero kwa Mulungu! Pafupifupi zakasikisite zapitazo ine ndinalandira Iwo.”85 Tsopano, ngati iye akanakhala mphongolo, iye akanati,“Tsopano, dikira miniti, ine ndinatsimikiziridwa ndipondinakonkhedwa pamene ine ndinali…Chabwino, ndithudi,ndipo iwo anandilowetsa ine mu tchalitchi ndipo ndinampatsira

Page 18: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

18 MAWU OLANKHULIDWA

kalata yangawakuti.” Oh, chifundo ine! Iwo samadziwa nkomwekuti iwo ndi andani.86 Koma iye amadziwa kumene ufulu woyamba kubadwakwake umachokera. Iye anali pamenepo pamene izozinkachitika. Iye anabadwa mwa madzi ndi Mzimu. Iyeankadziwa, ndipo madzi kudzera mu kusambitsidwa kwa madzimwa Mawu, umatenga Mawu.87 Tsopano penyani momwe akuyankhulira izi, “Kwa iwoamene ali mwa Khristu Yesu.” Paulo, tsopano, kumbukirani…Ine ndikutenga nthawi yaitali, koma ine sindimaliza mutu uwu.Koma ine ndifulumira…Kodi inu mukuzikonda izi? Oh, Iwoakutiuza ife pamene ife tiri, koma ife sitingathe kuchita izo muusiku umodzi wokha. Ife tikusowekera mwezi umodzi kapenaiwiri ya izi, usiku uliwonse, basi kumangopita kudutsa Iwo,Mawu ndi Mawu. Kubwerera mmbuyo ndi kukazisakatula izokuchokera mu mbiriyakale ndi kudzaziyala izo, Mawu ndiMawu, ndi kudzakuwonetsani inu kuti Icho ndi Choonadi.Tsopano mundilole ine ndiwerenge ndime imeneyo mwachangukenanso.

Paulo, mtumwi wa Yesu Khristu mwa chifuniro chaMulungu (osati chifuniro cha munthu), kwa oyeraamene ali mu Efeso, ndi (mlumikizi) kwa okhulupirikamwa Khristu Yesu:

88 Zikutanthauza, “Iwo ayitanidwa atuluke, alekanitsidwa,ndipo tsopano abatizidwa mwa Mzimu Woyera, ndipo alimwa Khristu Yesu. Ine ndikulembera kalata iyi kwa inu,okondedwa anga.” Oh! Ine ndikuganiza za Paulo kumenekoali ndi iwo tsopano, oh, ndine wokondwa bwanji! Mtumwiwakale wamng’ono uja mutu wake unadulidwa kumusi uko.Ine ndinaima pafupi ndi malo amene iwo anamudula mutuwake. Koma, oh, mutu wake uli pa thupi la tsopano ilo, ndiposungadulidwenso nkomwe. Ndipo iye waima pamenepo ndi iwominiti yomwe ino, mtumwi yemweyo amene analemba Izi. Ndipoanati, “Kwa inu amene muli mwa Khristu Yesu! Mwa Mzimuumodzi ife tonse timabatizidwa kulowa mu Thupi limodzi ili.”Tsopano penyani.

Chisomo chikhale kwa inu, ndi mtendere, kuchokerakwa Mulungu Atate athu, ndi…Ambuye Yesu Khristu.Wodala ndi Mulungu ndi Atate wa Ambuye wathu

Yesu Khristu, amene watidalitsa ife ndi zonse…Oh, iwe ukumva zimenezo, Charlie?…amene watidalitsa ife ndi madalitso onse

auzimu…89 Osati kungoti ena kwa atumwi, ndi ena kwa ichi, komaIye watidalitsa ife ndi madalitso onse auzimu. Mzimu Woyerawomwewo umene unadzagwa pa Tsiku la Pentekoste ndi

Page 19: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 19

MzimuWoyera womwewo pano usikuuno. MzimuWoyera umeneunamupangitsa Maria kufuula ndi kuyankhula ndi malirime,ndi kukhala ndi nthawi yopambana ndi kukondwerera, ndizinthu zimene iye anachita, ndi Mzimu Woyera womwewopano usikuuno. Mzimu Woyera womwe uja umene unamulolaPaulo pa ngalawa yakale ija, pamene zinkawoneka ngati iyoyadzazamadzi ndipo ikumira, ndipomasiku fortini ndimausiku,kopanda mwezi kapena nyenyezi. Iye anayang’ana kunja ukondipo funde lirilonse linali ndi mdierekezi pa ilo, akuyang’ana,ndi kumanyezimiritsa mano ake, ndipo anati, “Ine ndikumizaiwe,mnyamatawakale, tsopano. Ine ndakupeza iwe tsopano.”

90 Ndipo pamene Paulo anatsikira mmusi kuti akakhalendi kapemphero kakang’ono, pamenepo panadzaima Mngelo,anati, “Usawope, Paulo. Ngalawa yakale iyi ikaphwasukirapa chisumbu chinachake. Kazipita ndipo ukadye chakudyachamadzulo chako, izo zikhala bwino tsopano.”

91 Apa iye akubwera ndi unyolo wakale uwo mmanja akeaang’ono okalamba, akukwakwaza iwo pa mapazi ake, ndipoanati, “Khalani olimba mtima, amuna, pakuti Mulungu, MngelowaMulungu, amene ine ndiri wantchitowake, anaima pafupi ndiine ndipo anati, ‘Paulo, usawope ayi.’” MzimuWoyera womwewouli pano usikuuno, Mzimu waMulungu womwewo, ukutumikirakwa ife madalitso auzimu omwewo.

…anatidalitsa ife ndi madalitso onse auzimu mmaloa mmwambamwamba…

92 Oh, tiyeni tiime miniti inanso apa. “Mmalo aMmwambamwamba.” Tsopano, basi osati kungokhalakulikonseko, koma mmalo a Mmwamwamba. Ifetasonkhana “Mmwambamwamba,” zimatanthauza kutimalo a wokhulupirira. Kuti, ngati ine ndapemphera, inumwapemphera, kapena mpingo wapemphera, ndipo ifenkukhala okonzekera Uthenga, ndipo tadzisonkhanitsa tokhapamodzi ngati oyera, oyitanidwa atuluke, obatizidwa ndi MzimuWoyera, odzazidwa ndi madalitso a Mulungu, oyitanidwa,osankhidwa, kukhala pamodzi mmalo a Mmwambamwambatsopano, ife ndi a Mmwambamwamba mu masolo athu.Mizimu yathu yatibweretsa ife kudzalowa mu chikhalidwe chaMmwambamwamba. Oh, m’bale! Ndi zimenezotu, chikhalidwecha Mmwambamwamba! Oh, chingachitike ndi chiyaniusikuuno, chingachitike ndi chiyani usikuuno ngati ife tikanatitikukhala pano mu chikhalidwe cha Mmwambamwamba, ndipoMzimu Woyera ukuyendayenda pa mtima uliwonse umenewakonzedwanso ndipo wasanduka cholengedwa chatsopanomwaKhristu Yesu? Machimo onse atakhala pansi paMagazi, mukupembedza kwangwiro, manja athu atakwezedwa mmwambakwa Mulungu ndipo mitima yathu itakwezedwa, titakhala

Page 20: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

20 MAWU OLANKHULIDWA

mmalo a Mmwambamwamba mwa Khristu Yesu, tikupembedzalimodzi mmalo a Mmwambamwamba.93 Kodi inu munayamba mwakhalapo mwa amodzi? Oh, inendinakhalapo mpaka ine kumalira ndi chimwemwe ndikuti,“Mulungu, musandilole konse kuti ndichoke pano.” Basikungokhalammalo aMmwambamwambamwaKhristu Yesu!94 Kutidalitsa ife ndi chiyani? Machiritso auzimu,kudzodzedweratu, vumbulutso, masomphenya, mphamvu,malirime, kutanthauzira, nzeru, chidziwitso, madalitsoonse a Mmwambamwamba, ndi chimwemwe chosanenekandi wodzaza Ulemelero, mtima uliwonse utadzazidwa ndiMzimu, kumayenda limodzi, kumakhala limodzi mmalo aMmwambamwamba, opanda lingaliro loipa lirilonse pakatipathu, opanda ndudu imodzi yosutidwa, opanda chovalachachifupi chimodzi, opanda ichi, icho kapena chinacho,opanda lingaliro loipa limodzi, opanda winawake wokhala ndimangawa pa wina ndi mzake, aliyense kumayankhula mwachikondi ndi mwachiyanjano, aliyense ndi mtima umodzi pamalo amodzi, “kenako mwadzidzidzi pamenepo panadzabwerakuchokeraKumwamba nkokomo ngati mphepo yankuntho.” Ndizimenezotu, “Watidalitsa ife ndimadalitso onse auzimu.”95 Kenako Mzimu Woyera ukhoza kugwera pa winawake,ndikuti, “PAKUTI ATERO AMBUYE. Pita ku malo ena akendipo ukachite chinthu chinachake.” Muwone icho chikuchitikabasi monga chomwecho. [M’bale Branham akukhwatchitsachala chake—Mkonzi]. Mukuona? “PAKUTI ATERO AMBUYE.Ukachite chinthu chinachake pa malo ena ake.” Muchiwoneicho chikuchitika basi monga choncho. [M’bale Branhamakukhwatchitsa chala chake].96 “Watidalitsa ife limodzi mu madalitso onse aMmwambamwambammalo aMmwambamwamba.” Penyani!

Monga momwe iye watisankhira ife…97 Kodi ife tinamusankha Iye, kapena Iye anatisankha ife?Iye anatisankha ife. Liti? Usiku umene ife tinamulandira Iye?Anatisankha!

Monga momwe iye anatisankhira ife mwa iye mazikoa dziko lapansi asanakhazikitsidwe, kuti ife tidzakhaleoyera…opanda chilema pamaso pa iye mwa…(zipembedzo?)…mu chikondi:

98 Ndi liti limene Mulungu anatisankha ife? Ndi litilimene Mulungu anakusankhani inu amene muli ndi MzimuWoyera? Ndi liti limene Iye anakusankhani inu? Mazikoa dziko lapansi asanakhazikitsidwe. Mwa kudzodzeratuKwake, Iye anakuwoneranitu inu ndipo anadziwa kuti inumukanadzamukonda Iye. Ndipo asanakhalepo maziko adziko lapansi, Iye anakusankhani inu, ndipo anamutumiza

Page 21: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 21

Yesu kuti Iye adzakhale chitetezero cha machimo anu, kutiadzakuitanireni inu ku chiyanjanitso, kwa Iyemwini, kuchikondi. Oh, ndikanakonda tikanakhala ndi nthawi yamaminiti angapo owonjezera.99 Ndiloleni ine, ife tisanapite patsogolo paliponse, ndibwereremmbuyo, Genesis 1:26. Ine ndidzazitenga izo Lachitatu. PameneMulungu anamupanga munthu…Iye asanamupange munthu,Iye ankadzitcha Iyemwini “El,” E-l, El; E-l-h, “Elah,” “Elohim.”Liwulo limatanthauza, mu Chihebri, “wokhalapo-yekha,” zonsemwa Iyemwini. Palibe chimene chinakhalapo Iye asanakhalepo,Iye anali wokhalapo yekha amene anakhalapo, Uyo wokhalapo-yekha! El, Elah, Elohim, amatanthauza “wokwanira muzonse, wamphamvu-zonse, Wamphamvuzonse, Uyo wokhalapo-yekha.” Oh!100 Koma mu Genesis 2, pamene Iye anamupanga munthu, Iyeanati, “Ine ndine,” Y-a-h-u, J-u-v-u-h, Yahweh, “Yehova.” Kodiizo zimatanthauza chiyani? “Ine ndi Uyo wokhalapo yekhayoAmene ndinalenga chinachake kuchokera mwa Inemwini,kuti chidzakhale mwana wa Ine, kapena wongoyembekezera,kapena wamng’ono, wachichepere wa Ine.” Ulemelero! Bwanji?Iye anamupatsa munthu…Yehova amatanthauza kuti Iyeanampatsa munthu kuti adzakhale mulungu wamng’ono.Chifukwa Iye ndi Mulungu Atate, ndipo Iye anamupangamunthu kukhala mulungu wamng’ono, chotero Iye si wokhalapoyekhanso, Iye akukhala ndi banja Lake. Elah, Elah, Elohim.Tsopano, tsopano Iye ndi Yehova. Yehova, kutanthauza,“Mmodzi Amene akukhala ndi banja Lake.” Tsopano, Mulunguanamupanga munthu kuti adzakhale wolamulira pa dzikolapansi lonse, iye anali ndi ulamuliro. Ndipo dziko lapansi linaliulamuliro wa munthu. Kodi limenelo ndi Lemba? Ndiye ngatiumenewo uli ufumu wake, iye anali mulungu pa dziko lapansi.Iye amatha kuyankhula, ndipo zimakhala chomwecho. Iyeamatha kuyankhula ichi, ndipo chimachitika chomwecho. Oh!Ndi Ameneyotu, Mulungu, Yehova, Mmodzi Amene anakhalapomu kukhalapo yekha, koma tsopano akukhala ndi banja Lake,ndipo ndi ana Ake limodzi ndi Iye. Ndi zimenezotu.101 Tsopano, mukawerenge zimenezo. Ife tidzalowa muzimenezo Lachitatu usiku, pamene ife tidzakhale ndi nthawiyambiri. Ife tangotsala ndi maminiti fifitini ena owonjezerandipo ife ti…Ine ndimaganiza kuti ndifika pamalo ena ake apa,koma ife sititero, kufika pamene ife tasindikizidwa ndi MzimuWoyera wa lonjezo. Chabwino.102 Tsopano, kodi ife tinaitanidwa liti kuti tidzakhale antchitoa Mulungu? Ndi liti limene Orman Neville anaitanidwa kutiadzakhale wantchito waMulungu? Oh, mai! Izi zimandipangitsaine kudzandima. Ine ndikuuzani inu, tiyeni titenge Malembaena. Ine ndikufuna inu mupeze Petro Woyamba 1:20. Ndipo, Pat,

Page 22: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

22 MAWU OLANKHULIDWA

upeze Chivumbulutso 17:8. Ndipo ine ndipeza Chivumbulutso13. Tsopano ife tikufuna kuti timvetsere apa, inu mukufuna kutimudziwe kuti ndi liti limene Mulungu anakuitanani inu kutimudzakhale Mkhristu. Oh, ine ndimazikonda izi. Izi, “Munthusadzakhala moyo ndi mkate wokha, koma ndi Mawu onseamene atuluka kuchokera mkamwa mwa Mulungu.” Chabwino,M’bale Neville, inu mwapeza Petro Woyamba 1:20. [M’baleNeville akuti, “1:20.”—Mkonzi]. Chabwino, muwerenge 1:19 ndi1:20. Mvetserani kwa izi. [“1:19 ndi 20.”] Inde. [M’bale Nevilleakuwerenga Petro Woyamba 1:19-20].

Koma ndi magazi ofunika a Khristu, monga amwanawankhosa wopanda chirema ndi wopandabanga:Amene ndithudi anadzodzedweratu

asanakhazikitsidwe maziko a dziko lapansi, komaanawonetseredwa mu nthawi zotsiriza izi kwa inu.

103 Ndi liti limene Iye anadzodzedweratu? Maziko a dzikolapansi asanakhazikitsidwe. M’bale Pat, ndiwerengereni ineChivumbulutso 17:8. [M’bale Pat akuwerenga Chivumbulutso17:8—Mkonzi].

Chirombo chimene iwe unachiwona chinalipo, ndipopalibepo; ndipo chidzakwera kutuluka kuchokera mudzenje lopanda malire, ndi kudzalowa ku chitayiko:ndipo iwo okhala padziko lapansi adzadabwa,amene maina awo sanalembedwe mu bukhu la moyochikhazikitsireni cha maziko a dziko lapansi, pameneiwo adzawona chirombo chimene chinalipo, ndipopalibepo, ndipo komabe chiripo.

104 Nndani ati adzanyengedwe? Nndani ati adzanyengedwe ndimunthu wachipembedzo uyu monga anachitira Sauli? Izo zinalizothyathyalika kwambiri chabe ndi zangwiro kwambiri mpakaizo zikanadzanyenga chiyani? Kumene Wo-…[Osonkhanaakuti, “Wosankhidwa.”—Mkonzi]. kukanakhala…[“kotheka.”]kukanakhala kotheka. Chabwino, Chivumbulutso 13:8, ndiloleniine ndikuwerengereni inu.

Ndipo onse amene akukhala pa dziko lapansiadza…onse amene akukhala pa dziko lapansiadzamupembedza iye, amene maina awo sanalembedwemu bukhu la moyo wa Mwanawankhosa wophedwaasanakhazikitsidwe maziko a dziko lapansi.

105 Maina athu anaikidwa liti mu Bukhu la Moyo waMwanawankhosa? Pamene Mwanawankhosa anaphedwamaziko a dziko lapansi asanakhazikitsidwe. Pamene Mulunguanali Yehova, El, Elah, Elohim, wokhalapo Yekhayo. Mongangati Diamondi imodzi yaikulu, ndipo Iye sakanakhalachinachakenso, koma mkati mwa Diamondi iyi zikhumboZake zinali Mpulumutsi. Mu zikhumbo izi, mkati mwa

Page 23: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 23

Iye, munali Mchiritsi. Chabwino, panalibepo kanthu kotiakapulumutse ndipo panalibe choti achichiritse, komazikhumbo Zake zinabereka izo. Chotero, ndiye maziko adziko lapansi asanakhazikitsidwe, pamene Iye ankadziwa,kuwonetsera kwakukuru apa kwa Iye, kuti Iye akanadzakhalaMpulumutsi, kuti Iye akanadzabwera ndi kudzasandulika thupindi kudzakhala pakati pathu, ndipo Iye ankadziwa kuti ndimikwingwirima Yake ife tikanadzachiritsidwa, Iye anaphaMwanawankhosa pa Bukhu Lake maziko a dziko lapansiasanakhazikitsidwe, ndipo analemba dzina lanu pa Bukhulimenelomaziko a dziko lapansi asanakhazikitsidwe. Oh!

106 Mvetserani kwa Ichi! Kukonzedweratu kumayang’anammbuyo ku kudzodzedweratu, ine ndikutanthauzakusankhidwa. Kusankhidwa kumayang’ana mmbuyo kukudzodzedweratu, ndipo kukonzedweratu kumayang’anakokafikira. Musaiwale zimenezo, kuti kusankhidwakumayang’ana mmbuyo apa, ndi izi apa, “Ine ndinali chisoso.Ine ndinabadwa mu tchimo, ndinaleredwa mu kusaeruzika,ndinabwera ku dziko lapansi ndikuyankhula mabodza,ndinabadwa pakati pa ochimwa. Abambo ndi amayi ndibanja langa lonse, ochimwa. Ine ndinali chisoso. Koma,mwadzidzidzi, ine ndinadzakhala njere ya tirigu. Izo zinachitikamotani?” Izo, ndi chiyani chimenecho? Kusankhidwa. Mulungu,maziko a dziko lapansi asanakhazikitsidwe, anasankha kutichisoso chidzakhala njere ya tirigu. “Tsopano ine ndikudziwandine njere ya tirigu, chifukwa ine ndinapulumutsidwa. Inendimachita motani izo?” Ndimayang’ana mmbuyo ndipondimawona kuti Iye anakonzeratu izo, kalekale. Mwakudzodzedweratu Iye anawona kuti ine ndikanadzamukondaIye, chotero Iye anakonza chitetezero kudzera mwa MwanaWake Yemwe, kuti kudzera mwa Iye ine ndidzathe kuchoka kuchisoso kupita kudzakhala njere ya tirigu. “Tsopano, kodi inendiri pati tsopano?”Ndinewopulumutsidwa, ine ndikuyendamuchisomo cha Mulungu. “Kodi kukonzedweratu kumayang’anachiyani?” Kokafikira. “Kodi Iye adzanditengera ine kuti, ndipokodi ine ndikupita kuti?” Ameni. Izo zakufikanipo inu. Ndizimenezotu.

107 Tsopano tiyeni tiwerenge mopitirira patsogolo pang’ono,ndipo kenako ife tiyenera titseke posakhalitsapa.

Monga mmene iye…anatisankha ife mwa iye mazikoa dziko lapansi asanakhazikitsidwe, kuti ife tidzakhaleoyera…opanda chilema pamaso pake mu chikondi:

Atatha kutikonzeratu ife ku kukhazikitsidwa,kukonzedweratu ku kukhazikitsidwa kwa ana mwaYesu Khristu kwa iyemwini, mogwirizana ndi kufunakwabwino kwa chifuniro chake,

Page 24: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

24 MAWU OLANKHULIDWA

108 Kodi Iye anachita chiyani? Iye, mwa kudzodzedweratu,anatiwona ife, akudziwa kuti Iye anali Mpulumutsi, wokhalapo-yekha. Kunalibepo Angelo, kunalibe kalikonse; kunangokhalaMulungu, Elah, Elohim, Iye wokhalapo-yekhayo, kunalibekalikonse koma Iye yekha. Koma mwa Iye munali Mpulumutsi.Chabwino, kodi Iye adzapulumutsa chiyani, kunalibekokanthu kalikonse kamene kanataika? Podziwa zimenezo,ndiye Iye anadziwa kuti chikhumbo chachikulu ichi mwaIye chikanadzatulutsa chinachake kutali uko chimene Iyeakanadzachipulumutsa. Kenako pamene icho chinachitachimenecho, mwa kudzodzedweratu Iye anayang’ana pansindipo Iye anamuwona aliyense amene akanadzavomereza Iwo.Ndiyeno pochita zimenezo, Iye anati, “Kuti ndipulumutse icho,njira yokhayo imene ndingachitire izo, ikhala kutsika pansiInemwini ndi kudzasanduka thupi ndi kukatenga tchimo lamunthu pa Iye, ndi kumufera iye, kuti Ine ndidzakhale Mmodziamene azidzapembedzedwa,” chifukwa Iye ndi Mulungu,chinthu chopembedzedwa.109 Kenako Iye anadzatsika pansi ndipo anadzadzitengerapa Iyemwini. Ndipo pamene Iye anachita zimenezo, Iyeanachita zimenezo kuti Iye adzakupulumutseni inu amenemukufuna kupulumutsidwa. Kodi inu mukuwona chimeneine ndikutanthauza? Mwa kudzodzedweratu, Mulunguwopandamalire, Amene ankadziwa zinthu zonse, anamuwonaMwanawankhosa, ndipo Iye anamupha Mwanawankhosayomaziko a dziko lapansi asanakhazikitsidwe, ndipo Iye anaikadzina lanu mu Bukhu la Moyo wa Mwanawankhosa. Ndipo Iyeanawona chinyengo cha Satana, chimene iye akanati adzachite.Chotero Iye anaika dzina lanu mmenemo. Ndipo Iye ananenakuti wotsutsakhristu adzakhala wachipembedzo kwambiri,wabwino kwambiri, munthu wabwino chomwecho, munthuwanzeru chomwecho, munthu wachipembedzo chomwecho,mwakuti iye akanadzanyenga osankhidwa kumene ngatikukanakhala kotheka. Koma izo ndi zosatheka, chifukwamaina awo anadzodzedweratu maziko a dziko lapansiasanakhazikitsidwe. Mwa kusankha Iye anawasankha iwo,ndipomwakukonzedweratu iwo amadziwa kumene iwo akupita.Ndi zimenezotu.110 Tsopano, nndani angakaikire zimenezo? Izo ndi zimenePaulo amanena. Amenewo ndi Malemba a Paulo. Zimenezondi zolemba za Paulo. Izo ndi zimene ankawuphunzitsampingo wake. Mpingo, unaikidwa pamalo, maziko a dzikolapansi asanakhazikitsidwe. Pamene Mulungu, mu ululu Wakewakubala, anali kubala, ankakubweretsani inu, akudziwazimene inu mukanadzachita, Iye anakuikani inu pamalo anu muThupi Lake Lomwe, kuti mudzakhale mkazi wapanyumba, kutimudzakhale mlimi, kuti mudzakhale mlaliki, kuti mudzakhalemneneri, kuti mudzakhale ichi kapena icho. Iye anakuikani

Page 25: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 25

inu pa malo anu. Kenako pamene ife tinabwera kuchokeraku maiko a gariki ku Igupto, kudzera mu kuyeretsedwa,ndipo nkubatizidwa kukalowa mu dziko lolonjezedwa…Pakuti, lonjezo la Mulungu ndi Mzimu Woyera. Aefeso 4:30,anati, “Musawukhumudwitse Mzimu Woyera wa Mulunguumene inu munasindikizidwa kufikira tsiku la chiwombolo.”Kenako Mulungu, atatha kuwukonzeratu mpingo, Iye anati,“Ndipo anthu onse, adzakhalapo mamillioni kuchulukitsamamillioni amene ati azidzayenda mwachipembedzo ndipoadzanyengedwa.” Okhawo amene sadzanyengedwa adzakhalaiwo amene awolokera mu dziko lolonjezedwa, amene maziko adziko lapansi asanakhazikitsidwe anali maina awo ataikidwamu Bukhu la Moyo wa Mwanawankhosa, ndipo adzalowamdziko lolonjezedwa, ndipo akusangalala nalo ilo.

111 Anthu ambiri amawopa kuti achita mowonjeza. Anthuambiri amawopa Mzimu Woyera ukupangitsani inu kuchitachinachake chimene inu—inu mudzachite nacho manyazikwa anthu. Anthu ambiri amawopa kuti alira, ndipowokondedwa wawo awawona iwo akulira, kapena amayi,kapena woyandikana naye wanu, kapena abwana anuakuwonani inu.

112 Mundilole ine ndikuuzeni inu za munthu nthawi ina,ndisanatseke. Panali mwamuna dzina lake Davide, ndipopamene likasa la Mulungu linali liri ku dziko la Afilisiti, ndipoIlo limabwera, likukokedwa ndi likasa, ng’ombe yokalambaimawakoka iwo, pamene Davide anawona likasa limenelokuti likubwera, iye anali atavala mkanjo waung’ono paiye, iye anathamangira kumeneko, anamenyetsa mapazi akem’mwamba, ndipo analumphalumpha, ndipo anakuwa ndikulumpha, ndipo anavina ndi kulumpha ndipo anavina. Ndipo,iye, ali mfumu ya Israeli! Ndipo mkazi wake anadzayang’anakudzera pa zenera ndipo anamuwona iye akuchita mwachilendokwambiri, iye anamunyoza iye. Bwanji, iye ayenera kutiananena kuti, “Chidempete! Tamuwonani iye uko, momweiye akuchitira, mmene akuponyera mapazi ake m’mwamba,ndi kumalumphalumpha pamenepo ndi kumachita mongachomwecho. Bwanji, ayenera kuti wapenga!” Ndipo usikuumenewo pamene iye anadzalowa, iye anati, molankhulachonchi, “Bwanji, iwe wandichititsa ine manyazi. Bwanji, iwe,wokhala mfumu, mwamuna wanga, kunja kuja kumachitachonchija, kumachita chonchija!”

113 Davide anati, “Mawa ndidzachita bwinoko kuposa pamenepaja. Inde, bwana!” Iye anati, “Kodi iwe sukudziwa kuti inendimavinira Ambuye?” Iye anali atawoloka! Iye anali ali mudziko la lonjezo. Iye anali atataya za kudzimva-yekha zonsezondi matope a mdziko. Iye anali wokondwa kwambiri atadziwakuti likasa linali kubweramumzindawakewomwe.

Page 26: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

26 MAWU OLANKHULIDWA

114 Ndipo, oh, ndikukuuzani inu, anthu ena amawopa kutialandire Mzimu Woyera, amawopa kuti ayamba kuyankhula ndimalirime. Iwo amawopa kuti winawake akhoza kunena kuti,“Tsopano, iye ndi mmodzi wa anthu a zamalirime aja.” Iwoamawopa kuti abwere ku tchalitchi ndi kudzabatizidwa muDzina la Yesu Khristu, chifukwa chakuti iwo akuchita nalomanyazi Ilo. Uh! Oh!115 Winawake akunena kuti ine ndikuyenera kutindikawachotseko matepi anga, chifukwa chakuti ndinalinditalalikira za kubatizidwa mu Dzina la Yesu Khristu. Inesindikukawachotsako iwo. Ine ndikupanga ochuluka! Ukonkulondola, kuti, ndikupanga ochuluka! Iwo ndi Baibulo. Ngatiiwo sakuzikonda zimene ife tinachita dzulo, mungopenyetsetsazomwe titi tipange mawa! Ndicho chinthu choti tizichita,mwaona, kumangoyendabe chitsogolo. Palibepo kuti iwoasiyika, chifukwa iwo ndi Ambuye. Iwo ndiMulungu.116 Inu mukudziwa chimene Mulungu anachita? Mulunguanayang’ana pansi kuchokera Kumwamba, Iye anati, “Davide,ndiwe mwamuna wa pa mtima Panga Pomwe.” Davidesamachita manyazi. Iye anali wantchito wa Ambuye. Iyeankawakonda Ambuye. Ndipo iye anali wokondwa kwambiri,anasangalala kwambiri, kufikira kuti sanaganizire za ulemererowa umunthu.117 Inu mukuona, monga ine ndinanenera mu ulaliki wangam’mawa uja, ife timachita mantha kwambiri, mpaka, kutitimafuna Saulo kuti atiphunzitse ife, ife timafuna ka Saulokochokera ku seminare inayake kuti kazitiphunzitsa ife momwetikuyenera kuchitira chipembedzo chathu ndi momwe ifetikuyera tizichitira izi. Zimenezo ndi tsidya linalo la Yordani.Tsidya lino, Mzimu Woyera ukutsogolera. Kuno inu mumakhalakuti mwachokamo mmatope amenewo. Kuno inu simusamalazimene iwo akuganiza. Kuno inu mwafa, ndipo moyo wanuwabisidwa mwa Khristu kudzera…ndipo wasindikizidwandi Mzimu Woyera. Inu simusamala. Inu mukukhala muKenani. Inu mukhoza kudya chimanga chabwino. Ndinucholengedwa chatsopano mwa Khristu Yesu. Inu mukupita kudziko lolonjezedwa.118 Ine ndikukumbukira nditaima uko, M’bale Collins,zaka zina sarte zapitazo, pamene tchalichi ichi chinalichisanamangidwe. Unali msonkhano waung’ono wa msasandinakhala apa pa ngodya, msonkhano wanga woyambirira. Inendinkalalikira Uthenga womwewu uwu, chinthu chomwechi,chuma chosafufuzika cha Khristu, ubatizo wa mmadzi muDzina la Yesu Khristu, kukhulupirira Mawu aliwonse kukhalaChoonadi, ubatizo wa Mzimu Woyera, machiritso Auzimu,mphamvu za Mulungu, chimodzimodzi basi monga momweine ndikuulalikirira Iwo tsopano, sindinachokeko nkomwe

Page 27: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 27

inchi imodzi kwa chirichonse cha Iwo. Mulungu waulululazochuluka za Iwo kwa ine, chotero, pamene Iye akuwulula Iwo,ine ndimangopitiriza kumawubweretsapo Iwo. Iye sachotsaponkomwe zimene zakhala ziripo, Iye amangokhala akupitirizakumawonjezera zochuluka pa Iwo.

119 Ine ndinaima kumusi uko pamene pafupifupi anthu faifihandiredi anaima pa gombe, akuimba, “Ndaima pa gombela nkuntho la Yordani, ndipo ndikuyang’anitsitsa, ndikupitaku Kenani dziko lokoma ndi lokondwa, kumene kuli chumachanga. Ndikadzafika ku malo athanziwo ndi kukadalitsikakwa nthawizonse, ndikadzafikako ndi kudzakhala ya Atateanga…ndi kudzapuma kwanthawizonse?” Pamene iwoanayamba kuimba imeneyo, ine ndinali ndikumutengeramnyamata kukalowa naye mu mtsinje kuti ndikamubatizeiye uko mu Dzina la Ambuye Yesu. Ine ndinati, “Atate aKumwamba, pamene ine ndikumubweretsa mnyamata uyu kwaInu pa kuvomereza kwake…” Ndiri mnyamata, inemwini,ndiri nazo zithunzi za izo kunyumba. Ine ndinati, “Pamenendikumubatiza iye ndi madzi, Ambuye, pa kuvomerezakwake, mu Dzina la Yesu Khristu Mwana wa Mulungu,Inu mumudzadze iye ndi Mzimu Woyera.” Ndipo pafupifupinthawi imeneyo Chinachake chinayamba kuzungulira, ndipoapa Icho chimabwera chikuzungulira kumatsikira pansi,Nyenyezi Yowala ya M’mawa inadzaima pamenepo. Pamenepopanadzaima Kuwala kuja kumene inu mumakuwona apo pachithunzi. Pamenepo Iko kunadzaima.

120 Icho chinapita kuzungulira dziko lonse, mpaka uko kuCanada ndi kozungulira. Iwo anati, “Kuwala kodabwitsakwawonekera pa mtumiki wamba wa Baptisti pamene iyeamabatiza.”

121 Masiku pang’ono apitawo, pamene Dokotala Lamsaanabwera kwa ine, ndipo samadziwa kalikonse ka izo, ndipoanandibweretsera ine chithunzi, chimene m’bale ali nachoicho uko tsopano. Kodi muli nacho chithunzi chija? KodiBaibulo uli nalo, chiri mmenemo, chiri mu bukhu lako?Chabwino. Pamenepo panali chithunzi cha chizindikiro chakalecha amakedzana cha Chihebri cha Mulungu, ndendendebasi chijachi chimene chinalipo m’masiku a Yobu, Baibulolisanalembedwe nkomwe. Mulungu ali mu zikhumbo zitatuZake, osati milungu itatu. Mulungu m’modzi mu zikhumbozitatu. Atate, Mwana, ndi Mzimu Woyera, maudindo atatuamene Mulungu anagwiriramo ntchito. Osati milungu itatu,zikhumbo zitatu! Ndipo Icho chinali pamenepo. Pamenemunthu wamkulu uja, Dokotala Lamsa, kumasulira kwaBaibulo la Lamsa, pamene iye ananena m’mawa umenewo.Pamene ine ndinamuuza iye zimenezo, ine ndinati—ine ndinati,“Chizindikiro chimenecho ndi chiyani?”

Page 28: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

28 MAWU OLANKHULIDWA

122 Iye anati, “Chimenecho ndi chizindikiro chamakedzanacha Mulungu, mu Chihebri. Mulungu, Mulungu mmodzi muzikhumbo zitatu.”

Ine ndinati, “Monga ngati Atate, Mwana, ndi MzimuWoyera?”123 Iye anaimikira, ndipo anakhazika kapu yake ya khofipansi, iye anandiyang’ana ine. Gene, ndikukhulupirira iwe unalipamenepo, Leo. Anati, “Inumukukhulupirira zimenezo?”

Ine ndinati, “Ndi mtima wanga wonse.”124 Iye anati, “Usiku wathawu, nditaima mu msonkhano wanu,M’bale Branham, ine ndinawona kuzindikira za mumtimakumeneko. Ine ndinali ndisanakuwonepo iko nkomwe muAmerika, mu dziko langa.” Iye anati, “Anthu achi Amerika awasamalidziwa nkomwe Baibulo. Chinthu chokhacho chimene iwoamachidziwa ndi chipembedzo chawo. Iwo samadziwa nkomwepamene iwo akuima.” Anati, “Iwo samadziwa chirichonse.”Iye anati, “Koma pamene ine ndinaima pamenepo usikuwatha,” anati, “ine ndinati…” Tsopano, M’bale Gene, inendikungonena izi molemekeza ndi chikondi ndi zotero. Iyeanati, “ine ndinati, ‘Ameneyo ayenera kukhala mneneri.’ Komapamene ine ndikuwona kuti inu mumakhulupirira kuti Atate,Mwana ndiMzimuWoyera siinalimilungu itatu, zinali zikhumbozitatu, ndiye ine ndadziwa kuti inu ndi mneneri wa Mulungu,kapena apo izo sibwenzi zitawululidwa kwa inu chomwecho.”Iye anati, “Chimenecho ndi chizindikiro changwiro.” Anati, “Inesindinayambepo…”Anati, “Inu si waumodzi?”125 Ine ndinati, “Ayi, bwana. Ine sindine waumodzi.Ine ndimakhulupirira mwa Mulungu kukhala MulunguWamphamvuzonse, ndipo zikhumbo zitatuzo ndi maudindoatatu chabe ameneMulungummodziyo anadzakhalamo.”126 Iye anati, “Adalitse mtima wanu!” Iye anati, “Tsiku linainu mudzakhetsera magazi anu padziko lapansi chifukwa chazimenezo, koma,” anati, “aneneri nthawizonse amafa chifukwacha ntchito yawo.”127 Ndipo ine ndinati, “Chotero izo zikhale chomwecho, ngatiizo zidzamukondweretsa Ambuye wanga.” Kumasulira kwaBaibulo la Lamsa.128 Oh, ndi zoona kwambiri. Ndi kangati, monga inendimanenera kwa mpingo uno, monga Samueli ananeneraiwo asanamusankhe Sauli, “Inu musanatuluke ndi kukajowinachipembedzo chinachake tsopano, ndi kukazimangirira nokhamu mtundu wina wa chipembedzo, bwanji osangowulola MzimuWoyera kuti uzikutsogolerani inu?” Bwanji inu osamutengaMulungu kukhala Mtsogoleri wanu ndi kumulola Iye kutiazikudalitsani inu, ndi kuyiwala za chipembedzo chanucho.Tsopano, ine sindikunena kuti inu musakhale wa chipembedzo

Page 29: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 29

chirichonse cha tchalitchi, inu mukhale wa chirichonse chimeneinu mukuchifuna. Izo ziri ndi inu. Koma ndikukuuzaniinu, ngati munthu panokha, mulole Mzimu Woyera kutiuzikutsogolerani inu. Inu muziwerenga Baibulo. Ndipo chimeneBaibulo likukuuzani kuti muchite, inu muzikachita chimenecho.Mulungu akudalitseni inu.129 Ndipo tsopano ine ndadikirira nthawi yaitali. Inendikudabwa ngati alipo aliyense pano yemwe amafunakuti abwere kudzadutsa pa mzere wa pemphero kutiadzapemphereredwe. Ngati alipo, angakweze manja awo.M’modzi yekha, awiri, atatu. Chabwino. Inu nonse mubwerekuno ndipo mudzaime apa ndiye ngati inu mukufuna kutero, panthawi ino, ndipo—ndipo tikhala ndi pemphero. Ndipo tikaterondife…ine sindikufuna kuti inu muchoke pakalipano. Inendikufuna kuti ndichite mwadongosolo chinachake pano basiife tisati—tisanatseke.130 Ndi angati amene akonda kuphunzira kwa Bukhu laAgalatiya…oh, ine ndikutanthauzaAefeso? Tsopano, Lachitatuusiku, ife tidzalowa mu Chisindikizo. Ndipo kenako Lamlungulotsatira mmawa, tidzakalowa mu kuwuika mpingo pa maloake. Oh, ngati…mwinamwake ife tidzayambira zimenezo,Lachitatu usiku likubwerali, kwa inu anthu kuno mu Jeff.Kuwuyika mpingo pa malo ake pamene iwo akuyenerakukhalapo, aliyenseyo. Momwe ife timaitanidwira mwakukhazikitsidwa. Mulungu watikhazikitsa ife kukhala ana,ndife ana mwa kubadwa. Tinakhazikitsidwa ndi kuyikidwa pamalo mwa Mzimu woyera. Taonani! Aliyenseyo anali Muhebri,pamene iwo ankawoloka mtsinje, koma Yoswa analigawadzikolo ndipo anampatsa aliyense malo ake monga mwazoyankhula za amayi ake pa kubadwa, kumene Mzimu Woyeraunkamuuza iye.131 Tayang’anani pa Yakobo pomwe iye ankafa, mneneri,wochititsidwa khungu, anakokera mapazi ake pa bedi, anati,“Bwerani kuno inu ana a Yakobo ndipo ine ndikuuzani inukomwe inu muti mudzakakhale pa tsiku lotsiriza.” Ulemerero!Oh, ine ndikudziwa ndikhoza kuwoneka mwachilendo.Anthu akhoza kuwoneka mwachilendo. Koma, oh, ngatiinu mukanangodziwa chi—chitsimikizo, ku—kuyaka kwa mumtima! “Bwerani kuno ndipo ine ndikuuzani komwe inu mutimudzakakhale mmasiku otsiriza.” Ndipo ine ndikhoza kutengaLemba lomwe lomwelo, ndi kutenga mapu a kumene Ayudaakukhala lero ndi kutsimikizira kwa inu kuti iwo ali pa maloomwewo amene Yakobo ananena kuti iwo akanadzakhala mutsiku lotsiriza. Ndipo sanachite konse, kumeneko, sanakhalepa malo amenewo kufikira iwo atadzabwerera kuyambirapa Meyi seveni, 1946, usiku umene Mngelo wa Ambuyeanawonekera kwa ine kumtunda uko ndipo nandiuza kutumauku. Ndipo ine ndikhoza kukuwonetsani inu zimenezo,

Page 30: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

30 MAWU OLANKHULIDWA

pamene iwo ankabwerera kupita mdziko latsopanolo, iwoamadzafikira ndendende pa malo amene Yakobo adanena kutiiwo akanadzakhalapo. Ndipo uko iwo akukhala pamenepo lero.Oh, oh, mai, oh, mai! Ife tayandikira ndi tsiku limodzi kufikaKwathu, ndizo zonse.132 Inu anthu okondedwa, amene mukudwala, kapena inusibwenzi mutaimirira pamenepo basi kufuna kungoti muime.Ndine m’bale wanu. Ndiri ndi kutuma kochokera kwa Mulungukuti ndidzapempherere odwala. Osati ngati zanga…ngati kutindiri ndi mphamvu yochiritsa, ine ndiribe. Koma ndiri ndimphamvu ya pemphero. Monga ine ndinanena mmawa uja,Davide analibe chirichonse koma legeni yaing’ono, koma iyeanati, “Ine ndikudziwa chimene iyo iti idzachite ndi mphamvuya Mulungu pa iyo.” Mukuona? Ine ndangokhala ndi pempherolaling’ono lokha kuti ndikupempherereni inu, ndi manjaanga kuti ndiwayike pa inu, koma ine ndikudziwa chimenechikhulupiriro mwa Mulungu chichite. Icho chawachitirapoena, icho chidzakuchitirani inu. Inu muzikhulupirira zimenezotsopano pamene inu mukunyamukapo, yandikirani pang’ono kumalowa.133 Tsopano, ine ndikudabwa, kuti ndizipange izi zikhalezokhudza, ngati ine sindingamupemphe m’bale wanga kutiabwere kuno ndi kudzawazodza iwo ndi mafuta. Kodi inumungachite zimenezo,M’baleNeville? Ine ndiwupemphempingongati inu mungaweramitse ku pemphero.134 Tsopano kumbukirani, sabata latha pamene ine ndinadwalakwambiri chifukwa cha mafuta akale a nsasi aja, inendikanakhoza kungololera chirichonse ngati winawake akanatiabwere ndikudzaika manja pa ine. Ngati ine ndikanakhalandi winawake atabwera pafupi, yemwe Mulungu wamudalitsandi kumuthandiza, ine ndikanayamikira izo kwambiri. Inunonse mukumverera tsopano monga mmene ine ndimamvererapamenepo. Inu mukumverera tsopano kuti mukufuna kutindikuchitireni monga mmene ine ndimafunira winawakekuti andichitire ine nthawi imeneyo. Mulungu asalole kutiine ndidzaizembe konse ntchitoyo. Ine nthawizonse, kayandatopa, kaya ndalema, pamene ine sindikukhoza kunyamulaphazi limodzi kuchoka pa limzake, ine ndizipita, chifukwa inendidzakakumana ndi aliyense wa inu kenanso, uko mu Dzikolija kumeneko.135 Ndiye inu akazi okalamba, amuna okalamba, olema, tsitsila imvi ndi lothothoka, ndipo likuthothoka mzidutswa mongaduwa limene latsegula kantibo kake, nkumagwetsa maluwaake ndi nkumathothokapo, inu mukungosweka mzidutswa,si choncho inu? Ndiko kulondola. Basi…Ndipo chinthuchokhacho chimene inu mukufunira kuti muzikhalapo ndikutimuziwala kwa ulemelero wa Mulungu. Chotero pamene mdani

Page 31: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 31

wakumbwandirani inu tsopano ndipo wakuthawitsani, inendikubwera ndi legeni ya Mulungu, ndi chikhulupiriro, ndimphatso imene Mulungu anandipatsa ine. Izi ndi zimeneine ndinanena, kuchitira kuti inu mumvetse izi. Ine ndinati,“Ngati Petro atati wangolowa, kapena ena a iwo.” Musanenezimenezo. Inu musachite kundipempherera ine. Mungolowamonga chonchi, ndipo mudzanene, monga kwa mkazi uyu,kuti, “Kodi ndinu mlongo Wakuti-ndi-wakuti?” Dzina lanundi ndani? Mlongo Howard. Kuti, “Ndinu Mlongo Howard.Ndinu wokhulupirira, Mlongo Howard? Mukukhulupirira.Ndinuwokhulupirira. Ndiye, inumukuona, muli ndi maufulu kumadalitso onse achiwombolo.” Ndiye ine ndikhoza kunena kuti,“Mlongo Howard, chirichonse chikhala bwino,” ndi kuchokapo.Oh, motani…ine ndinati, “Ine ndikhoza kufuula, ndikhozakukuwa.” Ine ndingati, “Ambuye, zikungoyenera kuchitika. Izozikungoyenera kuchitika.”136 Ndipo ine ndinaganiza, “Chabwino, anthu amaganizachinthu chomwecho pamene ine ndibwera kutindidzawapempherere iwo.” Chotero ndicho chimenecho.Mukuona chimene ine ndikutanthauza?137 Ndipo ine ndaimapo, nthawi zambiri, ndi kuwatenga anthu,ndi kuti, “Oh, mlongo wofunika, kodi inu mukhulupirira Izo?Oh, kodi inu mukhulupirira Izo?” “Ambuye, Oh Mulungu,apangitseni iwo kuti akhulupirire Izo. Muwapangitse iwoakhulupirire Izo.” “Oh, chonde, kodi muzilandira Izo tsopano?Si zimenezo ayi. Ine ndinazisiya zimenezo. Ine ndinachokako kuzimenezo.

Ine ndimangonena kuti, “Mlongo Howard, inu ndiwokhulupirira?”

“Inde, ndiri.”138 “Chabwino, Mlongo Howard, ngati ndinu wokhulupirira,ndinu wolandira wa chirichonse chimene Mulungu ali nacho.”Ndipo nkungomugwira dzanja lake. Mwaona, ndikukhulupirirazimenezo. Ine ndamukhudzaMlongoHoward poyikamanja angapa iye. Yesu sananenepo kuti “mukawapempherere iwo,” Iyeanati, “Akangoikamanja awo pa iwo.” Ndi zimenezotu, ndiye iyenkuchiritsidwa. Iye akhoza kunena kuti, “Chirichonse chikhalabwino,” Mlongo Howard. Ndiye mukhoza kupita kwanu ndipomukakhala bwino. Mulungu akudalitseni inu.139 Ndinu mlongo…[Mlongo akuti, “Hampton.”—Mkonzi].Mlongo Hampton, ndinu wokhulupirira, sichoncho inu?[“Ndine.”] Ndinu wolandira chirichonse chimene Iye anapereka.Mulungu akhale nanu, Mlongo Hampton. Mupite kwanu ndipomukakhala bwino tsopano. YesuKhristu akakuchiritsani inu.140 Ndinu mlongo…[Mlongo akuyankhula—Mkonzi].Slaughter. Ndizo…Ndinu amene tinakupemphererani kuchipatala. Ndinu wokhulupirira, ndiye, Mlongo Slaughter,

Page 32: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

32 MAWU OLANKHULIDWA

wolandira wa zonse zimene ife timazipempha. MlongoSlaughter, mulandire zimene inu mwazipempha, ndipomukakhale bwino. Mulungu apereka izo kwa inu.141 M’bale Gene, inu mukukhulupirira kuti Mulunguakupatsani inu? [M’bale Gene akuti, “Inde, bwana. Inde,bwana.”—Mkonzi]. Ndipo Ambuye Mulungu akupatseni inu,Gene, ndendende chimene inumwachipempha!…?…142 Ine ndikukudziwani inu. [Mlongo akuyankhula—Mkonzi]. Ndinu wokhulupirira, mlongo. [“Oh, inde.”] Inendikukudziwani inu. Awa ndi amuna anu pamenepo. Ndiiyeyo amene ndinamupempherera pa foni tsiku lija. Inenthawizonse ndimakumbukira zimenezo. Sindinathe kupitaku msonkhano ku Tulsa. Anabwera ku msonkhano. NdipoAmbuye anamuchiritsa iye, ndinamutumiza iye ku msonkhano.Moimirira wina inu mukumuimirira winawake. [“Mphwanga.”]Ndi chinthu cha Chikhristu bwanji chimenecho, mlongo!Mukuona? Iye anadzakhala woimirira ena nayenso. Iyeanatiyimirira tonse a ife. Ndinu wokhulupirira ndipo mulindi ufulu kwa chirichonse chimene Mulungu anachilonjeza.Ndine wantchito Wake. Ndipo mu Dzina la Yesu Khristu,ine ndikukupatsani inu chomwe mwachipempha. [“Inendikukhulupirira izo.”]143 Bwerani, M’bale Neil. Mulungu akudalitseni inu. Wakhalawabwino modabwitsa kwa inu. Ndinu wokhulupirira.Ndikudziwa inu muli. Ine ndikukhulupirira kuti Mulunguakupatsani inu chirichonse chimene inu mukuchipempha,pakuti ndinuwokhulupirira. NdipomongawantchitoWake, kwainu, m’bale wanga, mu Dzina la Yesu Khristu, ndikukupatsaniinu chokhumba cha mtima wanu. Pitani ndipo mukalandireicho. Mulungu akudalitseni inu.144 Mlongo Bruce, ine ndikukudziwani inu. Namwinowamng’ono amene anakhula nsana wanga amakudziwaniinu. Iye amachokera kumusi uko pafupi ndi Motel JJ, TwinJ, kapena chinachake monga chimenecho. Inu muwaimiriraena. Ndipo kodi chokhumba chanu ndi chiyani usikuunokuchokera kwa Atate anu? [Mlongo Bruce akuti, “Cha inemwini,usikuuno.”—Mkonzi]. Cha inumwini, usikuuno. [Mlongo Bruceakuyankhulanso]. Ndiye, mdani wakugwedezani inu kuposamomwe dokotala angathere, koma ine ndikukutsatirani inu,ndi legeni. Ndipo mu Dzina la Yesu Khristu, ndikulunjikitsamuvi wa legeniyo pa mwala umene unakalowa mu impsyozomwe zatsekekazo. Izo zikubwezeretsani inu kwa Mulungu,ku nyumba Yake.

Ife takupemphani Inu, kudzera mu Dzina la Yesu Khristu.Ameni.145 Kodi ndinu bambo a mwamuna uyu, bwana? Kodi ndinuwokhulupirira? [M’bale akuyankhula—Mkonzi]. Chophuka

Page 33: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 33

mmbali mwanu; mmusi, ndipo kumanzere kwanu. Kodi inumukukhulupirira kuti Mulungu apereka izo kwa inu, bwana,ndipo monga wantchito Wake?146 Ambuye, dzanja ili mwinamwake lachita ntchito zambirizovuta za m’tsikuli. Wabwera pano ndi cholinga, chinachakechoti achichite. Perekani izo, chokhumba cha mtima wake,Atate, pamene ine ndikupemphera mu Dzina la Yesu kuti inumutero. Ameni.147 Musati mukaikire. Chophuka chimenecho chisiyakukupwetekani inu mmusi pamenepo, ndipo mukhala bwino.Mulungu akudalitseni inu m’bale.148 [Mlongo akuti, “Chimapweteketsa mutu wanga ndikummero kwanga. Chikumapweteketsa nthiti zangandikamakhosomola. Ine ndimalephera kuimba. Inendikumalephera kuchita chirichonse. Ine…?…Ndipondikumalephera kugona mokwanira. Ndikumalepherangakhale kuchita chirichonse.”—Mkonzi]. Ndinu wokhulupirira,sichoncho inu? [“Ndine. Ndine wodzadzidwa ndi MzimuWoyera.”] Ndinu wokhulupirira. [“Ine ndikudziwa kutiMulungu amakhala mkatimu.”] Ndipo ndinu wo—ndinuwolandira wa madalitso onse awa. [“Ine ndikudziwa. Ndipoine ndikukhulupirira. Ine ndimakhulupirira mu mapempheroanu, M’bale Branham. Ine ndikukhulupirira kuti Mulunguandichiritsa ine. Ine ndikukhulupirira kuti Iye amayankhamapemphero anu.”] Zikomo inu.149 Atate, ndikumubweretsa uyu, mlongo wanga, mu mzere wamoto, pa chirikati cha chandamale. Ndipo ine ndikumubwezeraiye kwa inu, kuchokera mu zikhadabo za mdani, mu Dzina laYesu Khristu. Ameni.150 Basi ndi momwe izo ziti zidzakakhalire. [Mlongo akuti,“Inde, M’bale Branham.”—Mkonzi].151 [Mlongo akuti, “…?…Ndiri ndi phapo limene limafa,ndipo limodzi linafa.”—Mkonzi]. Opareshoni yamapapo.152 O Ambuye, pamene mkazi wamng’ono uyu waimiriraapa, chonsecho ali pa kuphukira kwa unyamata, inendikumupempherera iye. Ndipo phapo limene limayenera kutilikachotsedwepo, ndipo iye adziwerama, moyo wake wonse.Ndinu Atate athu, ndipo ine ndikulunjikitsa moto wa pempheropa iye kumene, Ambuye, molunjika kupita ku phapo limenelo.Ndikutumiza pemphero ili mu Dzina la Yesu Khristu. Mulole ilolikakhudze phapo limenelo ndi kulichiza ilo. Mu Dzina la YesuKhristu, ine ndikupempha izi. Ameni.153 NdinuMlongo…[Mlongo akuti, “MlongoGibbs.”—Mkonzi].Mlongo Gibbs. [“Mmutu mwanu momwe, ndipo ndikumamvakupweteka pamenepo.”] Ndendende. Mutu wanu waweramira

Page 34: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

34 MAWU OLANKHULIDWA

kwa ine. Ndinu wokhulupirira ndi wolandira wa madalitso onsea Mulungu, Mlongo Gibbs.154 Ambuye, ine ndikumubweretsa iye kwa Inu, ndi legeniyaying’ono iyi imene Inu munandipatsa ine, monga momwemunamupatsira Davide legeni, kuti aziyang’anira nkhosaza abambo ake. Ndipo ngati mdani abwerapo kutsatirankhosa, iye sankachita mantha. Iye amatenga legeni yaing’onoiyo ndipo amaitsatira mikangoyo ndi—ndi zimbalangondo,ndipo amabwera nayo nkhosayo. Ili ndi pemphero lachikhulupiriro. Inu munandiuza ine kuti ngati ndingati“ndiwapangitse anthu kuti akhulupirire ndi kukhala owonamtima.” Ine ndikumubwezeretsa Mlongo Gert usikuuno. Inendikumulanditsa iye mmanja a mdani. Iye ndi nkhosa Yanu. Inendikumubwezeretsa iye ku khola la Atate, mu Dzina la YesuKhristu. Ameni.155 [Mlongo akuti, “Mlongo Lowe.”—Mkonzi]. Mlongo Lowe.[“Ine ndiri ndi vuto la kuthamanga kwa magazi.”] Kuthamangakwamagazi. Ndipo ndinuwokhulupirira, si choncho inu,MlongoLowe? Wolandira wa madalitso onse.156 Ndiye, Atate Mulungu, ine ndikulinga pemphero iliusikuuno, monga ngati lochokera ku legeni ya Mulungu, pakuthamanga magazi kwa Mlongo Lowe. Ndipo mulole kutinthawi ina imene dokotala adzamuyeze kathamangidwe kamagazi, mulole adzamuyang’ane iye ndi kuti, “Akuyenda bwinotsopano.” Iye adzadziwa chimene chachita izo. Mu dzina la YesuKhristu, ine ndikupereka izo kwa iye. Ameni.157 [M’bale akuyankhula ndi M’bale Branham—Mkonzi]. Inde.Ine ndikanakonda ndikanakhala ndi adadi anga pano usikuuno,ine ndikanawapempherera iwo pompano. Ine nditero kwa anu,aponso. Ine ndikumvetsa.158 Atate a Kumwamba, mwamuna amene ali kholo wamnyamata uyu, kuti iye ali pano pa dziko lapansi chifukwa chaiye. Ndipo mwana wake yemwe akukhumba kuti abambo akeabwezeretsedwe; ali kutali uko mu dziko la tchimo, chidakhwa.O Ambuye, ine ndikutumiza pemphero ili ndi chikhulupirirondi mphamvu, ndipo ndi zonse zomwe ndingaliponyere nazoilo, nsangalabwi yaing’ono iyi, mu Dzina la Ambuye Yesu. Inendikuwuvunga iwo pa mdierekezi uyo yemwe anaika chinthuchimenecho chimene chagwidwa uko. Ndipo mulole kuti ichochichoke. Ndipo mulole iye abwerere motetezeka ku khola, muDzina la Yesu. Ameni.159 [M’bale akuti, “Mundipempherere ine,M’bale Branham, kutindikhale ndi Mzimu Woyera. Ine ndikufuna kuti ndirandireMzimu Woyera. Ine ndikuyenera kutero. Ine ndiri nachochokhumba. Ine ndikuyenera kuti ndilandire Mzimu Woyera.”]Inu muli nacho chikhumbo choti muwulandire Iwo. MukufunakutimubweremuDziko kumene kulimalonjezo onse. [“Inde.”]

Page 35: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 35

160 Ndipo tsopano, Ambuye, mnyamata uyu ali kutsidya chabekwa mtsinje, wamanga msasa ku tsidya linalo, ndipo Yordaniakusefukira. Ndipo palibe njira iliyonse kuti iye angawolokepokhapokha Inu mutampangira njira monga Inu munachitirakwa Yoswa ndi kwa Israeli. Ndipo, Atate, ine ndikukupemphaniInu, ngati wantchito Wanu, mumulole m’bale wathu wofunikira,O Mulungu, mulole iye alowe mu Dziko lolonjezedwa ili, lonjezoili. Kuti, ku mbali inayo, monga ine ndinatengedwerako usikuwina uja, mundilole ine ndikakhale ndi mwayi womugwira iyendi kumukumbatira manja anga iye, mu Dziko lina ilo, nkuti,“M’bale wanga wofunika.” Perekani izi, Ambuye. Mulole iyealandire lonjezo laMulungu,MzimuWoyera. Ameni.161 O Ambuye, kwa uyu, m’bale wanga wachisomo; dzanja ililomwe lakhala lachifundo kwa ine, ndipo landichitira zinthuine, zimene ziri zosaneneka. Iye akukhulupirira ndipo ali ndichikhulupiriro. Ndipo tsopano mdani akuyesetsa kuti amugwireuyu, mzangayu; shuga; ndipo iye akuganiza kuti iye—iye akhozakumugwira mnyamata uyu. Koma ine ndikumutsatira iye.Ine ndikubwera, kudzamubwezeretsa Wanu yemwe, Ambuye,kuvunga mwala uwu ndi chikhulupiriro cholunjika. Mu Dzinala Yesu Khristu ine ndikukantha matenda a shuga awo!…?…m’bale wanga. Bwezeretsani nkhosa Yanu yomwe ku khola,Atate, mu Dzina la Yesu. Ameni.

[MlongoBell akuyankhula ndiM’bale Branham—Mkonzi].162 O Ambuye, mlongo wathu akudziwa kuti kunenepetsa ukundi kumeneku, chotero adokotala akuti, ndi chinthu chomwechidzakupheni inu. “Paundi iliyonse, kulemera kopitirira,kumakuchotsera chaka chimodzi,” monga mwa kalendala yainshuranse. Ndipo iye akufuna akhalire moyo kwa ulemu ndimatamando a kwa Mulungu. Ndipo palibe dokotala yemweangachite izi, Atate Mulungu. Izo zangokhala mu—mu dzanjaLanu. Ndipo Mlongo Bell wakhali ali wokhulupirika kwambiri.Ndipo wakhala ali wachifundo ndi womvetsetsa mmayesero,amene akudutsamo. Iye wadutsa mmayesero akuya ambiri.Ine ndikumutsatira iye usikuuno, Ambuye. Ndikubwera kutindidzakumane naye mdani ameneyo uko. Ine ndikulunjika ndikulondolera konse komwe ine ndingalunjike nako. Mu Dzinala Yesu Khristu ine ndikuvungira mwala uwo wachikhulupiriropa mdani uyu yemwe wamugwira iye. Mulole umubalalitse iye,ndipo umuthamangitsire iye kutali ndi iye, ndipo iye adzakhozekuti abwezeretsedwenso ku msipu wa mthunzi wobiriwira ndimadzi odikha, kudzeramwa YesuKhristu. Ameni.

Zichitika, Mlongo Bell. Musakaikire basi.163 Mlongo Spencer. [Mlongo Spencer akuti, “M’bale, M’baleBill, ine ndimawakonda Ambuye bwino tsiku lirilonse lomweine ndimakhala moyo. Ndipo ndakhala ndikubwera kuno kwazaka twente, pa malo ano. Ndipo ndakhala ndikuchiritsidwa

Page 36: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

36 MAWU OLANKHULIDWA

pafupifupi chirichonse chomwe chakhala chondivuta ine.Mukukumbukira zonse za izo, ndi…?…”—Mkonzi]. Inendithudi ndikutero, mlongo…?…[“Ndipo Iye wandidalitsaine kwambiri! Ndipo ine ndimamukonda Iye bwino, tsikulirilonse la moyo wanga. Ndikudziwa ine ndiri ndi moyowopambana mwa Ambuye.”] Ine ndikukhulupirira zimenezo,Mlongo Spencer. [“Ndine wokondwa. Ndine wokondwa! Ngatiuwu si Mzimu Woyera umene ine ndiri nawowu, ine ndi—inendikadali paguwabe pa chirichonse chomwe Iye alinacho kwaine. Ndipo ine ndidzafera paguwa.”] Ameni. [“Ndi pameneine ndimafunira chotsegulira chitseko, kuti ndifera paguwandi Yesu.”] Ameni. Mulungu, apereke izo kwa iye. Ameni.[“Ndipo ndikuuzani inu chimene ine ndikufuna kuti inumuchite. Ndipo ndiri panjira, ndinangotenga banja langalonse ndi ine. Koma ine ndikufuna banja langa lonse, inumukudziwa.”] Ine ndikumvetsa. [“Ine ndikufuna okondedwaanga apulumutsidwe.”] Ana anu. Ndiko kulondola. [“Ndi anaanga.”] Inde, amayi. [“Ndi nyumba yanga.”] Inde, bwana. Inendikudziwa zimenezo. [“Ine ndikumverera kuti iwo onse alibwino.”] Inde. [“Inumunatipempherera ife.”]164 Ife tonse tikumudziwa Mlongo Spencer, ndipo tikudziwamomwe iye ndi M’bale Jess atsalirabe kudutsa mu zowawa,koma iwo akhala akubwera ku tchalitchi kuno. Pamene inenditi ndidzawolokere ku tsidya linalo, iwo samadzakavutikakomonga chonchi. Iwo adzakakhala achichepere. Oh! M’bale Jess,ngati ine ndikanangoti…?…inu mukudziwa. Ndiyeno inunonsemukudziwamomwe, basi—kungowoloka pang’ono…?…kutsidyako, inu mukabwerera kukakhala mtsikana wamng’onokachiwiri, ndipo M’bale Jess akabwereranso kukakhalamnyamatawamng’ono.Mulungu anakulonjezani inu.165 Tsopano, taonani. Ine ndikufuna kuti ndikupatsenikuphunzitsa pang’ono chabe, pokhala kuti ndinu womalizirapano, ine ndikufuna kuti ndikupatseni.166 Chifukwa, ine ndikudziwa uyu ndi mnyamata wanuwamng’ono, Charlie. Inu mukufuna kuti iye apemphereredwe?[M’bale Charlie akuti, “Inde.”—Mkonzi].167 Ine ndikufuna kuti ndinene chinthu chimodzi ichi. Kodimunayamba mwawerengapo mu Lemba pamene Baibulolinanena izi? Paulo anamuuzaKenturiyowa Chiroma.

Inu mukukhoza kundimva ine bwino bwino? [Osonkhanaakuti, “Ameni.”—Mkonzi].168 Anamuuza wa Chiroma, pamene iye anasolola lupanga lake,kuti adziphe yekha, uko ku Filipi pamene iye anali mu ndende.Ndipo chivomezi chinagwedezera ndendeyo pansi. Iye anati,“Ukhulupirire pa Ambuye Yesu Khristu, ndipo iwe ndi nyumbayako mudzapulumutsidwa.” Kodi inu munayamba mwamvapozimenezo? [Osonkhana akuti, “Ameni.”—Mkonzi]. “Iwe ndi

Page 37: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 37

nyumba yako.” [“Ameni.”] Tsopano, taonani. Ngati iwe uli ndichikhulupiriro chokwanira cha chipulumutso cha pa iwemwini,kodi iwe sungakhale nachonso chikhulupiriro chokwanira chapa nyumba yako? [“Ameni.”] Mulungu, mwanjira inayake,achita izo.169 Ndipo, Ambuye, ine ndikumupempherera Mlongo Spencerndi M’bale Spencer, usikuuno, kuti mwana aliyense, iwo ndiana awo, onse akakhale mu Dziko laulemerero, lokondwa ilokumeneko kumene sikukakhalako matenda kapena ukalamba,kopanda chisoni kapena zokhumudwitsa, ndipo moyo wonsewawung’ono uwu pano udzazimirira mu maloto ameneanadutsa. Mulole iwo alandire ichi, ndipo mulole ana ake onse,ndi mwamuna wake, okondedwa ake onse, ndi onse ameneamamukonda iye, ndi onse omwe iye amawakonda, mulole iwoakakhale kumeneko ndi iye, muDzina la Yesu. Ameni.170 [Mlongo Spencer akuti, “Ameni. Zikomo inu.”—Mkonzi].Mulungu akudalitseni inu. [“Ine ndikhala eyite-thuu,posachedwapa.”] Zaka eyite-thuu zakubadwa. [“…?…Koma iwo amafooka, akafika usinkhu umenewo. Koma inendikumachitabe zophika zanga, kuchapa ndi kusita, ndikukonza m’nyumba.”] Basi monga momwe dziko likupasukira,Mlongo Spencer. [“Inde, ndi choncho. Ndikumakhala wotopakwambiri, nthawi zonse. Iwo amakhala nazo izo…Inendinawafunsa amayi anga, amayi anga ondipeza, omwe analindi zaka nainte zakubadwa, momwe iwe umamverera pameneiwe ukukalamba, kalekalelo. Iwo anati, ‘Rose, mwinamwake iweumakhala wotopa nthawi zonse.’ Ine ndatopa.”] Chabwino, iweumangokhala kuti wakonzekera kuti uzipita kukapumula, inumukuona. [“Ine ndimakhala wotopa kwambiri, nthawi zonse.Ine ndikufuna nditapumula. Ine ndikusowa chimenecho.”]Inde, mayi. [“Ndipo ine ndikufuna kuti ndikapumule mwaAmbuye, pansi pa mawondo anga. Chonse, chirichonse chimeneine ndikuchisowa.”] Inde. Ingosungani chikhulupiriro chanumolondola pa Iye, Mlongo Spencer, ndipo inumudzawolokerako.[“Ine ndikufuna ndidzafere paguwa, mu Dzina la Yesu.Ndi amene ine ndimafuna nditakamuwona, kufikira Iyeakamaitanabe.”] Ndipo Iye anati…[“Ine ndikufuna chirichonsechimene Iye wandisungira ine.”] Ndipo motsimikiza basi mongamomwe ine ndaimira pano chomwechi ndi inu, usikuuno,Mlongo Spencer, mwa chisomo Chake ine ndidzakakuwonaniinu ndi Jess kutsidya linalo, wamng’ono ndi wathanzi. Inu nonsemudzakhala mukuthamangirako, mukufuula, “M’bale wanga!M’bale wanga!” [“Inde.”] Inde ndidzakakuwonani inu.

Manjenje ake.171 Atate Mulungu, mtsikana uyu anali ndi kusokonezeka,ndipo iye wadutsa poti mankhwala sangamuthandize. Pali iyeyekha, amene akulepheretsa. Koma ine ndikumubwerera iye

Page 38: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

38 MAWU OLANKHULIDWA

usikuuno. Ine ndikubwera kwa Inu, Atate. Ine ndikubwera,kudzakupemphani Inu kuti mulondelere chipolopolo chimeneine ndikuyenera, nditi ndiwombere. Mulole icho chiwomberemolunjika, tsitsi lolukana kumbuyo kwake. Mulole pemphero ili,mu Dzina la Yesu Khristu, likakanthe manjenje amenewo ndipolikawakhudzulire iwo mzidutswa, ndikubwezeretsa nkhosa iyiya msipu wa Mulungu. Ameni.

Zikungoyera kutero, wokondedwa.172 [Mlongo akuti, “Mungopemphera. Ine ndiri ndi ana sikisiamene ine ndikumupempha Mulungu kuti awachiritse ndikuwapulumutsa.”—Mkonzi].173 Mulungu wa Kumwamba, perekani zimenezo, ana akesikisi amene iye akukhumba kuti apulumutsidwe. Iye wamvaumboni uja wa M’bale Daulton, ana ake aakazi okondedwa. Iyeakuwakhumba ana ake sikisi, Atate. Mulole iye akhale nawoiwo. Mulole iye adzakakumane nawo iwo mu Dziko ilo kumenekulibeko usiku, otetezeka bwino ndi ophimbidwa ndi Magazi aYesu Khristu. Ameni.

Mukhale nawo iwo, mlongo, pemphero langa.[Mlongoyo akuyankhula ndiM’bale Branham—Mkonzi].

174 Ine ndikukukhulupirirani inu. Palibepo chirichonse,nkomwe, chomwe chingathandizire izo. Iwo awapatsa iwokanthu kakang’ono komwe kakuwoneka ngati, oh, chinachakengati acetamin. Ndi cortisone, iwo amawatcha iwo. Awo, awoamakupha iwe, pafupifupi. Iwo amabalalitsa magazi akokwambiri. Koma, taonani. Mukuona, nyamakazi imakhalangati mkango umene unagwira nkhosa ndi kuithawitsira iyokutali. Tsopano, kodi legeni ingachite chiyani? Oh, mai! Apopali mkango waukulu, wobangula uli ndi mwanawankhosa.Ndipo iwo umakonda mwanawankhosa, chotero iwo wathawanaye mwanawankhosa. Koma Davide anatenga legeni ndipoanawutsatira iwo. Mukuona? Tsopano penyani. Iye anali ndimiyala faifi: f-a-i-t-h, iyemwini, m-w-a. Legeni yake inalim’dzanja ili: J-e-s-u-s. Iye amagenda mwakupha. Chinachakechikuyenera kuchitika. Tiyeni tiitsatire nyamakazi imeneyo,usikuuno,mwa pemphero ili. Mulungu apereke izo kwa inu.175 [Mlongo akuyankhula ndi M’bale Branham—Mkonzi].Iye akufuna kuti abatizidwe mu Dzina? [“Ayi. Ayi. Iyesananene zimenezo.”] Inu mukufuna kuti iye abatizidwe. [“Ndikhumbo langa kumuwona iye atabatizidwa.”] Zikomo inu,mlongo. Osati chifukwa chakuti imeneyo ndiye njira yake.Ndi chifukwa chakuti…Tsopano, ngati zimenezo zikanakhalamu Baibulo, za, “Atate, Mwana, ndi Mzimu Woyera,” ine—ine ndikanakhulupirira izo, ine ndikanakhala pomwepo ndiizo, mlongo. Ine—ine sindikanafuna kuti ndikhale wosiyanamulimonse. Ine—ine ndikanafuna kukhala chomwecho.Ine sindikanalola…ine—ine ndikayankhira zimenezo, inu

Page 39: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 39

mukuona. Ndipo ine ndikuyenera kunena izo basi m’mene Ilolikunenera izo; osati kuti ndikhalewosiyana, koma kuti ndikhalewowona mtima.176 Tsopano, Atate, ife tikutsatira okondedwa ake. Omwe alindi nyamakazi, ndipo apa iye akufuna kuti iye abatizidwe muDzina la Ambuye Yesu, pakuti pamenepo ndipo polowera pake.Ndicho chipata chotseguka. Ndi pamene Yoswa anatsegulaponjira imene imawolokera kupita ku dziko lolonjezedwa. Panalibemalo awiri kapena atatu amene anatsegulidwapo; analipoamodzi okha.177 Petro, pa Tsiku la Pentekoste, pamene Mpingounayambitsidwa koyamba, anaitsegula njira, anati, “Lapanialiyense wa inu ndipo mubatizidwe mu Dzina la YesuKhristu.” Iwo sanachokeko nkomwe pa njira imeneyo, aliyenseanawolokerapo kupita ku Dziko lolonjezedwa.178 Ena a iwo amayesetsa kuti awoloke, kumusi komwe ukokudzera pa kamtsinje kena, ndipo Paulo anati kwa iye, “Kodiinu munabazidwa ku chiyani? Kodi inu mukuyesera kutimuwolokere pati?”

Ndipo iwo anati, “Kumusi kuno kumene Yohaneanayang’anako.”179 Iye anati, “Chabwino, Yohane amangokulozerani inu kunthawi, ndi malo.” Ndipo kenako pamene iwo anamva ichi, iwoanabatizidwa pamtsinje woyenera. Ndipo iwo anawoloka, ndipoanakalandira MzimuWoyera, zabwino.180 Perekani izi kwa mlongo wathu ndi okondedwa ake, muDzina la Yesu Khristu. Ameni.181 M’bale Lyle. [M’bale Lyle akuti, “Ine ndikukhulupirira kutindithudi ndinu bwana woyenera, M’bale Branham.”—Mkonzi].Oh, m’bale! [“Munayendapo…?…Inu mukukumbukira ngatipakanakhala kuti mu loto, panabwera chinachake…?…Ngatiinu mulitchule lotolo, izo ndi zabwino. Awo ndi amene inendinali nawo. Chimene, inu nthawizonse mwakhala mukulotamolondola!…?…”] Inde. Apo ndi pakale. [“Inde.”] Inde.Ndine wokondwa…?…Mulungu akudalitseni inu. Inu mulipaulendo wopita ku Dziko lolonjezedwa tsopano! Mwinamwakeine ndichitchula chimenecho.182 Ndi angati akukumbukira basi utumiki uwuusanatsimikiziridwe kwa ine, ndipo ine ndikuwedza ndi munthutsiku lina, kumusi ku mtsinje uko, ku nyanja? Ndipo inendimagwira nsomba zing’onozing’ono, ndipo Mzimu Woyeraunabwera pa ine. Apo panali a…Bambo uyu ndi wa Mboniza Yehova, anali. Mchimwene wake ali pano penapake, BanksWood. Iye ali muno penapake, yemwe ali woyandikana nanewanga.

Page 40: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

40 MAWU OLANKHULIDWA

183 Uyu ndi Lyle. Ndipo anthu awa anali a Mboni zaYehova. Ndipo iwo anati, tsiku lina pamene ife tinkawedzakumusi uko, mnyamata uyu atatembenuka, ine ndinamuuzaiye kuti muli chinachake mmoyo wake, ndi chimene—chimenechinadzachitika, ndi zonse za izo. Zimene, iye wangondiuzakumene ine, ndipo tsopano wangozichotsamo izo mmoyomwake, uko nkulondola, zonse zomwe izo zinali. Zinalizolondola ndendende. Abambo ake ndi amene anali wo—wowerenga. Kodi adadi ali pano usikuuno, Billy? [Winawakeakuti, “Sindikudziwa.”—Mkonzi]. Ndipo iye ndi mkazi wake,awiri onse, anabatizidwa, kuchitira umboni mu Dzina la YesuKhristu, kuno mu dziwe. Ndipo mwamuna uyu anakhala pafupindi ine, tsiku lina.

184 Banks, ulikuti? Kodi iye ali pano usikuuno? [Winawakeakuti, “Kumbuyo komwe uko pa ngodya.”—Mkonzi]. Kumbuyopa ngodya. Inde.

185 Ndipo ife tinali tikuwedza. Ndipo, m’bale, mnyamata wangawamng’ono anali atapha…Ine ndimaganiza kuti iye analiatapha kamphaka, masiku angapo mmbuyo mwake. Mphakawa kholo wokalamba uja anali ndi gulu la tiamphaka, ndipoanakanyamula iko ndipo anakagwetsa iko. Ine ndinaganiza…ine ndinati, “Ambuye awukitsa moyo wawung’ono,” dzulo lake.Nkulondola uko, Lyle? [M’bale Lyle Wood akuti, “Inde.”—Mkonzi]. Atakhala uko ku una. Ndipo ine ndinati, “NdizoPAKUTI ATERO AMBUYE.” Ndipo ife tinawedza usiku wonsendipo sitinagwire kalikonse.

186 Mmawa wotsatira, ife tinali kuwedza, mmbuyo mu unawaung’ono, kuti tipeze ndunduma. Imeneyo ndi nsombayaing’ono. Ndipo M’bale Lyle anali ndi mtengo waukulu, ndipoiye anaisiya kuti ndunduma yaing’onoyo imeze iwo, mbedzayaikulu yomwe iye anali nayo, mpaka, pamene iye anaikokeraiyo panja, kachingwe kakang’onoko konse kanali kali pansi,mbedza yaikuluyo, m’mimba mwa ndunduma yaing’ono. Ndipopamene iye amaikokera iyo panja, iye amangoyenera kutiakokere panja matumbo onse ndi chirichonse kuchokera mundunduma yaing’onoyo, kuti aigwire iyo. Ndipo anangoikokeraiyo panja, chifukwa mbedza yaikuluyo inali itakodwa m’mimbamwa nsombayo. Ndipo pamene iye anatero, anaiponyera iyopansi mmadzi. Ndipo iyo inangonjenjemera, kanayi kapenakasanu, ndipo basi zinathera pomwepo, chifukwa matumboake ndi makha ake anali akulendwera kunja kwa kamwa yake.Ndipo iyo inayandama pamenepo kwa pafupifupi theka la ora,inadzayandamanso kubwerera pa timaudzu.

187 Ndipo ine ndinali nditakhala pamenepo, ndikuwedza. Ndipomwadzidzidzi, Mzimu Woyera unabwera, unati, “Yankhula kwansomba imeneyo.”

Page 41: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 41

188 Ine ndinati, “Nsomba yaing’ono, Yesu Khristuakukupatsanso iwe moyo wako.” Ndipo nsomba yaing’onoiyo, itagona yakufa mmadzi, inadzitembenuzira mbali yakeina, ndipo inangoti ruuuu, kukalowa m’madzi, mwaliwiro basimonga momwe iyo ikanathera.189 M’bale Lyle ndi M’bale Wood anali atakhala pamenepo.M’bale Lyle anati, “M’bale Branham, izo zinali za ine, chifukwaine ndinanena kwa yaing’onoyo…190 [M’bale Branham akuyankhula ndi M’bale Lyle Wood—Mkonzi]. Usikuuno, ine ndikhoza kuwauza iwo zomwe inumunanena? [M’bale Lyle Wood akuti, “Inu ndithudi mukhoza.Ziri bwino, M’bale Branham.”]191 Iye anati, pamene iye anatulutsa matumbowo mwa iyo,anaiponyera iyo pamenepo, anati, “Iwe wawombera chipolopolochako chomaliza, mzanga wamng’ono,” basi monga chomwecho.Anaiponyera iyo panja.

Iye anati, “Izo—izo zimatanthauza ine.”Ndipo ine ndinati, “Ayi,M’bale Lyle. Sizinali zimenezo.”

192 M’bale Banks kumbuyo uko, anati, “Ndi anthu angatimdziko lino, ndi masauzande angati, omwe angakonde kuimapamene ife tikuima pakali pano, kuwona mphamvu ya Mulunguikutsika ndikudzachita chinachake monga chimenecho!”Mwakuyankhula kwina, iye anali ngati…193 Ine ndikukhulupirira ife tonse tinamverera monga momwePetro anachitira, “Ndi zabwino kukhala pano. Tiyeni timangemakachisi atatu.” Mukuona? Uko nkulondola.194 Tsopano, M’bale Lyle, iwe wadzozedwa ndi Mzimu Woyeratsopano. Wachoka ku Igupto. Miphika ya gariki ndi nyansiza mdziko zatsalira mmbuyo. Iwe waima pa gombe laYordani tsopano, basi kutsidya ilo. Mulungu akuwolotsere iwekumeneko; Lyle.195 Mulungu Wamphamvuzonse, apa pali chikho Chanu. Iyendithudi anali mu kuzingwa kowopsya, Ambuye, koma mtimawanga unamutsatira iye. Mapemphero athu anangokakanthachibhakera chopangitsa nyenyezi kumeneko, ndipo chinthukumene chimene chimamumanga iye chamuchokera iye. Ichochaswedwa. Ndipo tsopano akuyenda kutsikira ku Yordani.[M’bale Lyle Wood akuti, “Zikomo Inu, Yesu.”—Mkonzi].Mtengereni iye ku Dziko lolonjezedwa, Ambuye. [“Inde,Ambuye.”] Ndipo mukamusindikize iye pakati pa anthu. [“Inde,Ambuye.”] Kuti, pa Tsiku laulemelero limenelo pamene ifetiti tidzakakumane kutsidya, mundilole ine ndidzamvererekukumbatira kwa mikono yake, akufuula, “M’bale wangawofunika!” [“Ameni.”] “Ine ndikumudziwa iye.” MumubweretseBanks limodzi ndi iye, Ambuye, mutero Inu; bambo ndi mayi,ndi onse a iwo, a chemwali, ndi banja lonse lalikulu ilo?

Page 42: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

42 MAWU OLANKHULIDWA

Mulole ife tonse tidzakakumane kutsidyako, Ambuye, ndipommodzi aliyense wa iwo adzadzidwe ndi Mzimu Woyera. InendikupempheramuDzina la Yesu. Ameni. [“Ameni.”]

Ine muwulandira Iwo, m’bale. Mulungu akudalitseni inu,M’bale Lyle.196 [Winawake akuti, “M’bale?”—Mkonzi]. Inde, m’bale. [“Palifoni imene ikuchokera kutali, ndi imfa, akudikirira pa lamya.”]197 Pali winawake akufa, pa foni yochokera kutali. Ndipondiperekamsonkhano kwaM’baleNeville ndikapitam’menemo.198 [M’bale Neville akuti, “Tsiku lopambana ndi lalikulu mwaAmbuye! Mulungu watichitira zinthu zina zopambana kwaife lero. Ziyembekezo zanga zakwaniritsidwa kwathunthu.”—Mkonzi].

[“Tiyeni tiime pamodzi, pa mapazi athu.]199 [“Mukumbukire msonkhano ndiye, Lachitatu usiku.Mukhale mukupemphera kwambiri. Mitima yonseyosakhutitsidwa, yosatsimikiza ilumikizane kwambiri ndiMulungu. ‘Nthawi yayandikira. Nthawi yake ndi ino. Lero ndirotsiku la chipulumutso.’]200 [“Mulungu adalitse aliyense wa inu alendo, anthu inu amenemukuchokera kutali. Pemphero lathu ndi, lakuti, Mulunguakupatseni inu zifundo za mayendedwe, kubwerera kumenemumakhala. Zinali zabwino kuti tinali nanu limodzi nafe. Ndipomuzitipempherera ife pamene mukupita, kuti Ambuye adalitsepa malo ano, aponso].201 [“Atate Athu Akumwamba, monga wantchito Wanuwabwera usikuuno, kudzagwira ntchito ya mu ofesi yawantchito Wanu ndi mneneri, kudzaimirira pakati, padanga,akupanga lingalo, akubwera kwa ife ndi chikhumbo choyakachawantchitoWanu,monga kubatizidwa ndiMzimuWoyera, ndikupatsidwa ofesi ya mneneri, kuti ayankhule kwa kam’badwokano. Mutithandize ife lero ndi usikuuno, kuti tilandire Uthengaumene ukubwera kwa ife, Ambuye, chirimbikitso, kuti tikhaleokonzeka.]202 [“Mumudalitse wina aliyense amene azidutsa pa makomo anyumba iyi usikuuno. Mulole matenda omwe ali pa ife, omwe ifesitikudziwa kalikonse ka iwo, mulole chisomo Chanu chodalandi mphamvu zitisamalire ndi kutitetezera ndi kutichizaife, ndi kutisunga ife, kufikira nthawi imeneyo pamene Inumudzakhale wokonzeka kuti mutisamutsire ife kupita ku mbaliinayo. Mudalitse onse ogwetsedwa ulesi ndi okhumudwitsidwa,amantha, ndi iwo amene ali ofooka.]203 [“Mulungu, ife tikupemphera usikuuno kuti mutiyenderemwapadera, kudalitsa kwa Mzimu Woyera, kuti kukhale pawapaulendo aliyense, mwendamnjira aliyense, mlendo aliyenseamene ali pa zipata zathu. Aliyense yemwe ati atuluke pakhomo

Page 43: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 43

usikuuno, mulole chotchinga cha Magazi icho, ochokera pamtandawaKalvare, aphimbemokwanira ndipo apereke.]

204 [“Mutichize ife pamene tikudwala. Mutisunge ife pafupi ndimphamvu Yanu yaikulu. Mutidzozere ife ku utumiki. Mutiloleife tikayende mu chikondi, pamaso Panu, masiku onse a moyowathu. Ndipo ife tidzakutamandani Inu chifukwa cha izi, pakutiife tikupempha izi mu Dzina la Yesu Khristu ndi chifukwa chaIye. Ameni.]

205 [“Ndipo Mulungu akudalitseni inu. Ndipo ndife okondwakuti tinali ndi inu. Gwiranani chanzawina ndimzake.”]

206 [M’bale Branham akubwerera pa nsanja pamene osonkhanaakugwirana chanza ndi kulonjerana wina ndi mzake pameneakuchoka.]

207 [M’bale Branham akuyankhula ndi winawake.]Ndikuyamikira kwenikweni zonse zimene inu mwandichitiraine, khadi ndi…?…Inde, bwana. Ndikuyamikirakwenikweni…?…

208 [M’bale Branham akuyankhula ndi M’bale Neville—Mkonzi.]Chotero ife tinatumiza mwala wa chikhulupiriro…?…Panalimwamuna wochokera konkuno…?…Chotero ine ndinatumizapemphero lomutsatira iye, mu Dzina la Yes Khristu. Wakhalaatagona pamenepo kwa ora, osagunda, osapuma, osapangachirichonse. Osapuma, osagunda, osatulutsa mpweya, osapangachirichonse; maso atakhala pa mutu wake, anadzagwerapaguwa. [M’bale Neville akuti, “Iye anangomusiya agonepamenepo kufikira pemphero limenelo litabwerapo.”]

209 Kodi ichi chikadali chotsegulabe? [M’bale Neville akuti,“Inde, ndi choyatsabe,” akulozera kuti maikrofoni akadalioyatsabe—Mkonzi].

210 Kodi ndingakhale ndi tcheru chanu? Kuntunda uko,mvangeri wamng’ono, mlaliki, kuno ku Indiana, amalalikira,anadzagwa ndi kufera paguwa, pafupifupi ora lapitalo.Pamene iye amalalikira, anagwera chafufumimba, ndipoanafera paguwa, mvangeri wodziwika, amalalikira kuno kuIndiana. Abusa anangobwera ndipo anadzandiimbira ine. Iyeanafa pamene amalalikira pansi pa kudzodza kwa Mzimu,anagwera chafufumimba, maso ake atakhazikika, kupumakwake kunamuchokera iye. Iye analengezedwa kuti wafa,wakhala atafa kwa ora. Ndipo chinachake chinawauza iwo kutiayimbire ku tchalitchi ndi kundipempha ine kuti ndipemphere.Chotero ine ndinatumiza pemphero kuti amubweze iye,mu Dzina la Ambuye Yesu. Mulumikizane nane mwachikhulupiriro, kuti lisaphonye chandamale; amutsitsimutse iyendi kumubwezeretsanso iye. Zikomo inu.

Page 44: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

44 MAWU OLANKHULIDWA

211 Mulungu akhale nanu, mpaka ndidzakuwoneninsoinu Lachitatu usiku. Inu anthu ochokera ku Georgia ndikozungulira, bayi-bayi. Mulungu akhale nanu.212 M’bale Branham akuchoka pa maikrofoni ndipoakuyankhula ndi ena, koma zoyankhulana zawo sizikumveka—Mkonzi].

Page 45: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

KUKHAZIKITSIDWA 1 CHA60-0515E(Adoption 1)

MAULALIKI A KUKHAZIKITSIDWA

Uthenga uwuwaM’baleWilliamMarrion Branham, unalalikidwamuChingereziLamlungu usiku, Meyi 15, 1960, ku Branham Tabernacle mu Jeffersonville,Indiana, U.S.A., unatengedwa kuchokera pa matepi ojambulidwa ndi maginitonudindidwa mosachotsera mawu ena mu Chingerezi. Kumasulira kwa Chichewauku kunadindidwa ndi kugawidwa ndi Voice Of God Recordings.

CHICHEWA

©2020 VGR, ALL RIGHTS RESERVED

VOICE OF GOD RECORDINGS, MALAWI OFFICE

P.O. BOX 51453, LIMBE, MALAWI

VOICE OF GOD RECORDINGS

P.O. BOX 950, JEFFERSONVILLE, INDIANA 47131 U.S.A.www.branham.org

Page 46: CHA60-0515E Kukhazikitsidwa 1 VGR · 2 MAWUOLANKHULIDWA kuphunzitsa kwa Baibulo kawirikawiri kumakhala… Inde, M’baleWelch,inebasi…ndimakuyang’anayang’anaiwe,ine

Chidziwitso kwa ofuna kusindikiza

Maufulu onse ndi osungidwa. Bukhu ili mukhoza ku printa kunyumba kwanu ngati mutafuna kuti mugwiritse ntchito inuyo kapena kuti mukawapatse ena, ulere, ngati chida chofalitsira Uthenga wa Yesu Khristu. Bukhu ili simungathe kuligulitsa, kulichulukitsa kuti akhalepo ambiri, kuikidwa pa intaneti, kukaliika pakuti ena azitengapo, kumasuliridwa mu zinenero zina, kapena kugwiritsidwa ntchito ngati njira yopezera ndalama popanda chilolezo chochita kulembedwa ndi a Voice Of God Recordings®.

Ngati mukufuna kuti mumve zambiri kapena ngati mukufuna zipangizo zina zimene tiri nazo, chonde mulembere ku:

Voice of God RecoRdinGsP.o. Box 950, JeffeRsonVille, indiana 47131 U.s.a.

www.branham.org